Sura ya 16

1 Nakambila vichito ivi kuti msadakoza kuipichidwa. 2 Siakuchocheni kubwalo kwa masinagogi, zene nthawi ikujha iyo kila uyosiwakupheni siwaganizile kuti wachita nchito ya bwino kwa ndande ya Mulungu. 3 Siakuchitileni vichito ivi kwa ndande siamjhiwa tate penancho siaijhiwa ine. 4 Nakambila vichito ivi kuti nyengo ukafika wayaya kuchokela, simkoze kuyakumbukila ndi ntundu umo wakukambilani mkoze anyiiwo. Sinidakukambileni kukuza vichito ivi kuyambila mmayambo kwa ndande nidali pamojhi namwe. 5 Ingakale chipano nipita kwa yujha wadanituma, nampho palibe mwa anyiimwe uyowanifuncha, "upita kuti?" 6 Kwa ndande nanena mau yaya kwa anyiimwe; chisoni chajhala mmitima mwanu. 7 Ata chimwecho, nikukambileni zene: ni bwino kwa anyiimwe nikachoka. Kwa mate ngatisinichoka otondoza siwajha kwanu, nampho nikapita sinimtume kwanu. 8 Wakala mmeneyo otondoza kuchimikizila jhiko kulingana ndi machimo kulingana ndi malinga ndi kulingana ndi malamulo. 9 Kulingana ndi machimoo kwa ndande siadanikukupalile ine, 10 kulingana ndi malinga kwa ndande nipita kwa atate, ndi simnionancho. 11 Ndi kulingana ndi malamulo kwa ndande wamkulu wa jhiko lino walamulidwa. 12 Nilinayo yambili ya kukukambila, nampho simzindikila chipano. 13 Nampho, iye mzimu wa zene, wakajha, siwakuchogoleleni muzene yonche, pakuti siwakambancho kwa chifuko chake mwene; nampho waliyenche siwayavele, siwayanene yochitika yameneyo, ndi kuyachinikiza kwa anyiimwe yochitika yayo siyajhe. 14 Iye siwanikuze ine, kwa ndande siwayatenge yochitika yanga ndi kulalikila kwanu. 15 Vindhu vonche alinavo atate ndi vayine, kwa icho, ninena kuti mzimu siutenge vochita vanga ndi kuyachimikiza kwanu. 16 Ikali ntawi yaifupi simunionancho, ndi pambuyo pa ntawi ya iupi, simunionancho. 17 Akumojhi wa opunzila wake adamunchana, "ndichiyani ichowatikambila," ntawi yaifupi simunionancho, ndi , ndipo ntawi ya ifupi simunione, "ndi kwa ndande nipita kwa atate?" 18 Kwaicho adanena, "ndi chindhu chanji ichowanena, ikali ntawi yaiupi?" Sitijiwa umowanenela. 19 Yesu wadanena kuti adakumbila kumuncha ndiiye adakambila, "mjhifuncha mwachinawene kukuza ili, umowanenela ikali ntawi yaifupi simunionencho, ndi pambuyo pa ntawi ya iupi simunione?" 20 Zene zene, nikukambilani, simulile haikudandaula, nampho jhiko silikondwele, simkale ndi chisoni nampho chisoni chanu siching'anamukile kukala chimwemwe. 21 Wamkazi wakala ndi chisoni nyengo yapowakala ndi vopweteka kwa ndande nyengo ya kujhimasula yoika, nampho yapowajhimasula mwana, siwakumbukilancho vopweteka kwa ndande ya chimwemwe chake kuti mwana wabadwa pajhiko. 22 Ninyi pia mna huzuni sasa, lakini nitawaona tena; na mioyo yenu itafurahi na hakuna atakayeweza kuiondoa furaha yenu. 23 Siku hiyo hamtaniuliza maswali. Amin, Amin, nawaambia, Mkiomba lolote kwa Baba, atawapa kwa jina langu. 24 Mpaka sasa hamjaomba lolote kwa jina langu; ombeni, nanyi mtapokea ili kwamba furaha yenu ikamilike. 25 Nakamba nsi anyiimwe kwa mkambo osajhiwike, nampho nyengo ikujha yapo sinikamba kwa mkambo osajhiwike nampho pambuyo pake sinikukambileni poyelayela kukuza Atate. 26 Siku limenelo simpemphe kwa jhina langa, ndi sinikukambilani kuti sinipemphe kwa atate kwa chiuko chanu; 27 Pakuti atate wene akukondani kwa ndande mnikonda ine ndi kwandande mnikulupalila kuti nachoka kwa atate. 28 Nidachoka kwa atate ndi najha pajhiko penancho, nichoka pajhiko ndi nipita kwa atate.'' 29 Opunzila wake adamkambila, upenya, chipano ukamba poyelayela ndi siuchita kwa vindapi. 30 Chipano tijhiwa kuti ujhiwa vichito vonche ndi siufuna mundhu waliyenche akuunche mauncho kwa ndande iyi tiikulupilila kuti uchoka kwa mulungu. 31 Yesu asawayankha, "chipano mwakulupalila?" 32 Penyani, nyengo ikujha yetu ndi chiichimichimi yaika, pamene simjhisonghaniche kila mmoji kwake kwake simunisiye namwene. Nampho sinilindeka kwa ndande atate alipamojhi ndiine. 33 Nikukambilani vichito ivi kuti mkati mwanga mkale ndi mtendele. Pajhiko mli ndi mavuto, nampho jipacheni mtima, nalikoza.