1 Usidavomeleza umoyo wako kukala pakati pohangaika, umulolela Mulungu munilolele ndiine. 2 Pakati panyumba yatate wanga pali ndi nyumba zambili zokala, ngati sidakakala mchimwecho, nidakala nakukambila, pandande nipita kukukonjelani pamalo pandande yako. 3 Ngati sinipite ndikukukonjelani malo, sindijejo kukukalibisheni kwanga ili pamalo nili pia namwe mkalepo. 4 Mujiwa njila pamalo ndipita." 5 Tomaso wadamkambila Yesu," Ambuye, sitijiwa kumalo ukoupita, bwa! Tikoza bwanji kuijiwa njila? 6 Yesu wadamkambila, "ine nde njila yauzene, ndi umoyo, palibe wakozae kujiwa kwa atate ingakale kupitila kwanga. 7 Ngati mudakalijiwa ine, mudakajiwa ndi atate wanga ndipo, kuyambila chopano ndikuendekela mujiwa ndikumuona iye." 8 ilipo wadamkambila Yesu, "Ambuye tilangize atate, ndichocho sivale yatukwana." 9 Yesu adamkambila sindidalipamoji nda nyiimwe kwandawi, yaitali, ndiukuli siundijiwa ine, ilipo? Walionje wamiona ine waona atate, khani yanji ukamba, tulangize atate? 10 Simuvananavo kuti ine ndimnyumba mwa atate, ndi atate ndi mnyumba mwanga? Mau ndiyakomba kwanu sindikamba padala langa namwene, pambuyo pake, ndi atate yao alama mnyumba mwanga yao achita njito yao. 11 Vananavo ine, kuti ndili munyumba mwa atate, ndi atate mnyumba mwanga, ndichocho muamini ine pandande ya njito zanga hasa. 12 Vananavo, vananavo, ndikukambilani iye wavananavo, ine njito zia nizichitazo, siwazichite nito izi pia, ndi siwachite ata njito zazikulu pandande ndipita kwatate. 13 Chilichonche simupembe pajina langa, sindichite pakuti atate akoze kukuzidwa, pakati pamwana. 14 Ngati simupembe chindu chilichonje pa jina langa, chimene sindichite. 15 Ngati simunikonde, simuyakwile malamulo yanga. 16 Ndi siniapembe atate, nao sakunikhe ni wakukutangatilani mwina ilikuti wakoze kukala pamoji namwe paufulu, 17 Loho yauzene. Jiko silikoza kumlandila iye pandande simumuona, pina kumuji wa iye, ata chochomwe mujiwa iye, pakuti wakala pamoji namwe ndisiwakale mnyumba mwanu. 18 Sindikusiani mweka, sindibwele kwanu. 19 Pandawi yaitali jiko silinionajo, nambo anyiimwe muniona, pandande muniona, pandande nitama, namwe simukale pia. 20 Pandawi imeneyo simukale kuti ine ndili mnyumba ya tate, ndikuti anyiimwe muli mnyumba yanga, ndikuti ine nili mnyumba yanu. 21 Walionje wangwila malamulo yanga ndi kuzichita, nde mmoji uyo wandikonda ine, ndi uyo wanikonda ine siwakondedwe nda atate wanga, ndi sinimkonde ndi sinilangize ine namwene kwake. 22 Yuda (apande Iskariote) adamkambila Yesu, "Ambuye, bwa! Ndichiyani chichokela kuti siujilangize umwene kwatu ndiopande pajiko?" 23 Yesu wadayankha ndikukwambila, "ngati walionje wanikonda, siwaligwile mau langa, atate wanga samkonde, ndisitipite kwake ndi sitichite makazi yatu pamoji naye. 24 Walionje uyo siwanikonda ine, siwagwila mau yanga. Mau ilo mulivela opande langa ndipo latate ilo anituma. 25 Nakamba vindu ivi kwanu, ndawi ni kali ndinikala pamoji namwe. 26 Atachocha, oniariji, umoyo wamtendele yao atate siamtume pajina, siwayaluze vindu vonje ndisakuchiteni mukambukile yonje yayo nidayakamba kwanu. 27 Mtendele nikunikhani mtendele wanu imwe. Sinikunikhani ii ngati jiko lichochavo nisidachita mitima yanu kukala ndi kuhangaika, ndikuopa. 28 Mdavela vicha nidakukambilani, nipita zanga, ndisinibwele kwanu! Ngati muda kunikonda ine, mudakakala ndi lahapandande nipita kwatate, pakuti atate ndi wakulu kupita ine. 29 Chopano nata kukukambilani popande kuchitika ichi kuti, ndawi sichichitike. mkoze kuvananavo. 30 Sindikamba namwe mau yambili, pakuti wamkulu wajiko lino, wabwela iye walibe mbavu pamwamba panga, 31 nambo ili kjti jiko lipate kujiwa kuti na konda atate, nichita icho nichita atate anituma ine, ngati umo aninikhila malamulo, imani, nditichoke pamalo pano.