1 Basi munthu mmoji jina lake Lazaro wadali odwala. Wadachokela ku Bethania, muji wa Mariamu ni dada wake Martha. 2 Wadali ni Marimu yuyuja wadampaka Ambuye mafuta ni kumpangusa myendo yake kwa machichi yake, ambaye m'bale wake Lazaro wadali ni odwala. 3 Ndeyapo dada anyiyawa adatuma utenga kwa Mpulumusi ni kukamba, "Ambuye, penyani yuja mumkonda wadwala." 4 Mpulumusi yapo wadavela wadakamba, "utenda umeneo osati wa kufa, chifuko chake ni kwa ndande ya ufulu wa Mulungu dala kuti mwana wa Mulungu wapate uulu katika umeneo utenda." 5 Mpulumusi wadamkonda Martha ni dada wake ni Lazaro. 6 Yapo wadavela kuti Lazaro ni odwala Mpulumusi wadakala siku ziwili kuendekela pamalo yapowadali. 7 Ndo baada ya ili wadakambila opuzila wake, "tieni Kuyahudincho." 8 Opuzila adamkambila, "amwalimu, Wayahudi amauna kuyesa kukubula myala, nawe ufuna kubwela kumenekoncho?" 9 Mpulumusi wadayankha, "saa za usana sizili kumi na mbili? Munthu yapo waenda usana siwakosa kujikwala, ndande wapenya kwa mwanga wa usana." 10 Ata chimwecho, ikakala waenda usiku, wajikwale kwa ndande mwanga palije mkati mwake." 11 Mpulumusi wadakamba vichito ivi, ni baada ya vichito ivi, wadakambila, "bwenji latu Lazaro wagona. Nampho nipita dala kuti nipate kumuucha kuchoka kulitulo." 12 Nampho opuzila adamkambila, "Ambuye, ngati wagona, siwauke. 13 Nthawi ii Mpulumusi wadali wakambilila nkhani za nyia ya Lazaro, nampho anyiio adaganize wakambilila nkhani yogona litulo. 14 Ndeyapo Mpulumusi wadakambila uzene, "Lazaro wafa." 15 Nili ni chisangalalo kwa ajili yanu, kuti sinidalipo kuja dala kuti mpate kukulupalila. Tieni kwa iye." 16 Basi, Tomaso watanidwa pacha, wadakambila opuzila achanjake, "nafe tieni pia tikafe pamoji ni Mpulumusi." 17 Nthawi Mpulumusi yapo wadaja, wadapeza kuti Lazaro tayari watokata mkaburi siku zinai. 18 Nayo Bethania idali pafupi ni Yerusalemu ngati kilomita arobaini tano chimwechi. 19 Ambili katika Wayahudi adaja kwa Martha ni Mariamu kwachezeche kwa ajili ya m'bale wao. 20 Ndekuti Martha yapo wadavela kuti Mpulumusi watokuja, wadapita kupezana naye, nampho Mariamu wadandekela kukala kukomo. 21 Ndeyapo Martha wadamkambila Mpulumusi, "Ambuye nati mdakakala pano, kaka wanga siwadakafa. 22 Ata saino, mjiwa kuti lalilonche mulipemphe kuchoka kwa Mulungu siwakupacheni." 23 Mpulumusi wadamkambila, "kaka wako ahyukencho." 24 Martha wadakambila, "mjiwa kuti wahyuke katika kunyakulidwa siku yotela." 25 Mpulumusi wadamkambila, "ine nde kunyakulidwa ni umoyo, iye wanikulupalila, ata chimwecho wakale walama; 26 Ni iyewalame ni kunikulupalila ine siwafa. Ukulupalila ili?" 27 Wadamkambila, "etu, Ambuye nikulupalile kuti iwe ni Mpulumusi, mwana wa Mulungu iye wakuja katika jiko lonche." 28 Yapo wadakamba ili, "wadachoka ni kumtana dada wake Mariamu kumphepete, wadakamba, amwalimu ali yapa ni akutane." 29 Mariamu yapo wadavela, wadaimuka mwa chisanga ni kupita kwa Mpulumusi. 30 Nae Mpulumusi wadali wadaji wakali mkati mwa kijiji, wadali wakali pamalo wadapezana ni Martha. 31 Ndeyapo Wayahudi wadali ni Mariamu katika nyumba ya anyiwaja adali amamtondoze, yapo adamuona waime chisanga ni kuchoka kubwalo, adamchata, adaganizo kuti wapita kukaburi dala wakalile kumeneko. 32 Ndi Mariamu, yapo wadafika paja Mpulumusi wadali wadamuona ni kugwa panchi pamyendo yake ni kumkambilani, "Ambuye ngati mdakali pano, mbale wanga siwadakafa." 33 Mpulumusi yapo wadamuone walila, ni Wayahudi adaja pamoji ni iye adali amatolila nao, wadadandaula katika mzimu ni kukosa mtendele. 34 Wadakamba, "mwamgoneka kuti? Adamkambila, Ambuye, majani mpenye." 35 Mpulumusi wadalila. 36 Nde yapo Wayahudi wadakamba, "penya umo wadamkondola Lazaro!" 37 Nampho wina kati ayo adakamba, "osati uyu munthuwadayatambasula maso ya yuja wadali osapenye, wadakoze kumchita uyu munthu wasafa?" 38 Ndeyapo Mpulumusi wadali wadandaula mumtima mwakencho, wadapita kuli kaburi chapano lidali jenje, ni mwala waikidwa pamwamba pake. 39 Mpulumusi wadakamba, "uchocheni mwala." Martha mlongo wake ni Lazaro, iye wafa, wadamkambila Mpulumusi, "Ambuye, kwa muda uno tupi likale laola, kwa ndande watokala chitanda kwa siku zinai." 40 Mpulumusi wadamkambila, "ine sinidakukambile kuti ngati ukakulupalila, siuwone ufulu wa Mulungu." 41 Kwa icho adauchocha mwala. Mpulumusi wadapenya maso yakekumwamba ni kukamba, "atate, niyamika pakuti munivela. 42 Nidajiwa kuti munivela nthawi zonche, nampho ni kwa ndande ya gulu ambalo laima kunizugulila kuti nayakamba yaya, dala kuti apate kukulapalila kuti iwe wanituma." 43 Baada yokamba yaya, wadalila kwa sauti yaikulu, "Lazaro, maja kubwalo!" 44 Wakufa wadachoka kubwalo wamangidwa manja ni myendo kwa nchalu zo zikila, ni kumaso kwake kudamangidwa ni kitambaa, " Mpulumusi wadakambila, "Mmasuleni mumsie wajipita." 45 Ndeyapo Wayahudi ambili anyiyao adaja kwa Mariamu ni kuona Mpulumusi wachichita, adamkulupalila; 46 nampho akumoji wao adapita kwa Maarisayo ni kwakambila ivo wavichita Mpulumusi. 47 Ndipo wakulu akulu anchembe ni Maarisayo adakusanyana pamoji katika pamalo nikukamba, "tichite chiani? Munthu uyu wachita malangizo yambili. 48 Ikakala timsia chimwechi iye yoka, onche siamukulupalile, Warumi siaje nikutenga vonche pamalo patu ni jiko latu." 49 Ata chimwecho, munthu mmoji kati yao, Kayaa wadali wa nchembe wa mkulu chaka chimwecho wadakambila, "simjiwa chalichonche kabisa. 50 Simganizila kuti ifai kwa chiuko chanu kuti munthu mmoji iunika kufa kwa chifuko cha wanthu kuliko jiko lonche kufa." 51 ya wadayakamba kwa chiuko cha mwene, pambuyo pake, pakuti wadali anchembe wamkulu chaka chija, wadalasa kuti Mpulumusi siwafe chiuko cha jiko; 52 Niosati kwa jikope toka, kuti Mpulumusi wapate mumuja kwakusenya wanaa Mulungu anyiyao apatuka malo ina ina. 53 Kwa icho kuyambila siku limenelo ni kuendekela adapanga umo ampele Mpulumusi. 54 Mpulumusi wadaendencho padanga kati ya Wayahudi, nampho wadachoka pamenepo ni kupita jiko lili pafupi popanda kanthu katika muji utanidwa Efraimu. 55 Basi Pasaka ya Wayahudi idali pafupi, ni ambili amakwela kupita Kuyerusalemu kubwalo kwa muji kabla ya Pasaka dala apate kujichocha chimo achinawene. 56 Adali kumfunafuna Mpulumusi ni kukamba kila mmoji yapo adali aime mkamba, "inganizila chiani?" 57 Muda uno wakulu akulu anchembe ni Maarisayo adali achoche lamulo kuti ikakala mmoji wajiwe Mpulumusi wali, ifunika kuchocha nkhani dala kuti apate kumgwila.