1 Mvanenavo mvanenavo ndikukambileni, yujosiwalowa kopitila chicheko chokala la mbelele. Nampho wakwela kwanjila ina yake, munthu mmeneyo ndi mnkhungu. 2 Iyo walowa mchicheko ndi oweta wa mbelele. 3 Kwake mlonda wa chicheko kumchukulila. Mbelele aivela sauti yake ndi kuzitana mbelele zake kwa majina yao ndi kwa choka kubwalo. 4 Yaposiachoche kubwalo ali wake siachogoze, ndi mbelele siwaachate,aijiwa sauti yake. 5 Siamchata mlendo nampho pambuyo pake. Siamuyepuke, pakuti siazijiwa sauti za ulendo. 6 Yesu wadakamba mfano huno kwao, nampho siadavielewe viatu niambavo wadali kuvikamba kwao. 7 Yesu wadakamba naoncho, "uvanenavo, uvanenavo nikukambileni, ine ndi chicheko cha mbelele. 8 Onche anyiao anichogolela ndi ankhungu ndi olanda nampho mbelele siwadavechele." 9 Ine ndi chicheko. Walienche siwalowe kupitila kwanga, siwaokoledwe. Siwalowe mkati ndi kuchoka, nae siwajipezele vakudya. 10 Mnkhungu siwaja ingakale kuba, mkumpa , ndikuteketeza, naja ilikuti apate umoyo ndi akaleno tele. 11 Ine ndi owesa wabwino. Owesa wabwino kuchocha umoyo wake kwa chifuko cha mbelele. 12 Mtumiki uyo siwasaukidwa, ndi asati owesa, iyembelele osati chuma chake, siaone agalu amtengo naaja ndi kuwasia ndi kuwatawa achimbelele. 13 Ndiagalu amtengo siagwile ndikuwatawanyicha. Kutawa kwachifuko ndi mtumiki kuajiliwa ndi siaganizila mbelele. 14 Ine owesa wabwino ndi nijiwa ali wanga nao ali wanga anijiwa ine. 15 Ambuye anijiwa nane najiwa Ambuye nane niuchocha umoyo wanga kwachiuko cha mbelele. 16 Nilimazo mbelele zambili ambazo osati za uzizi achaamene nao. Inifuna kwapeleka, nao saivele sauti yanga ilikuti pakalepo ndi kundi limoji ndi owesa mmoji. 17 Ichi chiuko ambuye anikonda. Ni uchocha umoyo wanga alafu niukwezancho. 18 Palibe wautenga kuchoka kwanga. Nampho niuchocha namwene. Nilinayo mamlaka.'' 19 Mgawanyikoncho udachokela pakati pa Wayahudi kwachifuko cha mau yaya. 20 Ambili wao adakamba wali ndi pepo ni ukichaa ndande yanji mumvenchela? 21 Wina adakamba, "yamene osati mau yamunthu wachanganyekiwa ndimapepo. Pepo likoza kuchakula maso yakipofu?" 22 Ndiyapo idaja sikukuu ya kuika waku Kuyerusalemu. 23 Idali nyengo yamphepo ndi Yesu wadali wamaendela hekalu katika nyumba ya Selemani. 24 Ndiyapo Wayaudi yapoadamzungulila ndikumkambila, "mpaka chakunji siutike mmavuto? Ngati iwe ndi Mkristo tikambile ukweli. 25 Yesu wadayankha! Natokukambila nampho simuniamini nchito nizichita kwanjina la Ambuye wanga nazo nizishuhudia pamwamba panga. 26 Ata chimwecho simuniani kwachifuko anyiimwe ojati mbelele zanga. 27 Mbelele zanga aivela sauti yanga namjiwa nao au ichata ine. 28 Naapacha uzima wa milele siangamiacho kamwe ndi palibe ata mmoji uyo siwanga kule kuchokela mmanja mwanga. 29 Ambuye wanga yaonipacha achameneo ndi wamkulu kuliko achameneo onche palibe ata mmoji wali ndi uwezo wakuwanyakula kuchokela mmanja mwa Ambuye. 30 Ine ndi Ambuye tu mmoji. 31 Adatenga myala ili amsinje ncho. 32 Yesu wadayankha, natokukulangizani nchito za mbili za bwino kuchoka kwa Ambuye kwa nchito ziti kati ya izi mfuna kunisinja myala. 33 Wayahudi adamuyankha sitikusinja myala kwa nchito yaliyonche ili yabwino. Nampho kwa kumphemphwa kwa chifuko iwe muntu ujichita kuti Mulungu. 34 Yesu wadayankha sidalembedwe kupitila lamulo lanu ndidakamba, "anyiimwe ndi miungo?" 35 Ikakala adawatana miungu kwa anyiwaja ambao mau la Mulungu lidajela ndi malembo siyakoza kuswedwa. 36 Mkamba pamwamba yuja ambaye adamchocha ndi kumtuma kupili kujiko uzalau kwa chifuko ndidakamba, "ine ndi mwana wa Mulungu?" 37 Ikakala sinichita nchito za ambuye wanga msidaniamini. 38 Ata chimwecho ikakala nizichita atangati simuniamini ziaminini nchito nchito ilikuti mkoze kujiwanchi kuzijiwa kuti ambuye wali mkati mwanga nchi iine nili mkati mwa Ambuye. 39 Adayesancho kumgwila Yesu nampho wadapita zake kuchokela mmanja mwao. 40 Yesu wadapita zakencho kung'ambo ya Yordani sehemu ambayo Yohana wadawi wamabatiza hati ndi kukala kumene. 41 Wanthu ambili adaja kwa Yesu adaendekela kukamba Yohana kweli siudachite ishara yaliyonchoche, nampho vinthu vonche wadavikamba Yohana pamwamba pa uyu muntu ndi ya uzene. 42 Wantu ambili adamwamini Yesu pamene.