Mutu 6

1 Manje pamene Saballati, Tobiah, na Geshemu mu Arabu naba dani batu bonse bananvela kuti na manga nafuti chibumba ndipo kunalibe gawo iliiyonse inasala yoseguka, ngakale sinenze nayika ziseko muzipata, 2 Sanballati na Geshemu banatumila ine nakukamba kuti, "Bwela, tiyeni tukumane pamozi mumalo yalibe kali konse ya Ono." Koma banali kufuna kuchita zoyipa kuli ine. 3 Ninatuma utenga kuli benve, nokamba kuti, "Nichiya nchito ikulu, ndipo siningabwele pansi. Nichani chito iyimilile nikachoka nakubwela pal kuli imwe?" 4 Bananitumila utenga wamene kwantawi zi 4, ndipo nibayanka mwamene ntawi iliyonse. 5 Sanballati anatuma kapolo wake kuli ine munjila yamene ntawi ya 5, nankalata yoseguka mumanja mwake. 6 Mukati yenze yolembewa, Ine "Nichokambiwa pakati ka chalo, na Geshemu nayenve akamba kuti, iwe naba Yuda mupulana ku panduka, ndiye chamene mumangila chibumba. Kuchoka mwamene malipoti akamba, iwe ufuna kunka mfumu yawo. 7 Wasanka baneneli kuti bapange ichi chilengezo mu Jerusalemu, kukamba kuti, "kuli mfumu mu Yuda!' Ungakale wosimikize mfumu aza nvela malipoti aya. Choncho bwela, tiyeni tikambe kani iyi pamozi." 8 Ndipo ninatuma mwau kuli enve kukamba kuti, "kulibe zintu zachichitika mwamene ukambila, chifukwa wavipangila mumutima wako." 9 Chifukwa bonse banali kufuna kuti ise tiyope benzoganiza, "manja yawo yazasiya nchito, ndipo nchtio sizachitika." Koma manje, Mulungu, Napapata limbisani manja yanga. 10 Ninayenda kunyumba ya Shamaya mwana wa Delaya mwana wa Mehetabeli, anali wosekeledwa munyumba mwake, "Tiyene tikumane pamozi munyumba ya Mulungu, mukati mwa tempele, ndipo tivale viseko va tempele, chifukwa ba bwela kukupaya. Usiku babwela kukupaya." 11 Nina yanka, "Nanga mwanuna alimonga ine angatabe? nanga mwamuna ali monga ine unga mu tempele kuti apulumuse umyo wake? Siniyenda mukati!" 12 Ninazindikila sana tumiwe na Mulungu, koma anali kunenela kusuna Ine. Tobiya na Sanaballati benze mugula. 13 Bana mugula kuti aniyofye, chakuti nichite vamene anakamba naku chimwa, chakuti banapase zina loyipa kuti anchite. 14 Itanani munzelu Tobiya na Sanaballati, Mulungu wanga kukonya namachitidwe yawo. Muyitane munzelu na muneneli Noadiya na bonse bannenli beanyesa kuniyofya. 15 Chibumba chinasila pa sika la twenti faivi mumwezi wa Eluli, patapita masiku yali fifite tu. 16 Pamene ba dani bonse bananvela, maziko yonse yanaliku kuti zunguluka, banayopa nakugwa maningi pamenso yawo. CHifukwa banali kuziba kuti nchito inachitwa nama tandizo ya Mulungu. 17 Pantawi iyi bolemekezewa ba Yuda banatuma nkalata kuli Tobuya, naba nkalata ya Tobiya yanabwela kuli benve. 18 Chifukwa banali bambili mu Yuda banali bo mangiwa na lumbiro kuli enve, chifukwa anali mupongozi mwamuna wa Shekaniya mwana wa Arah. 19 Mwana wake Jehohanani enzeli anatenga mukazi wokwatila mwana wa Meshulamu mwana wa Berechaya. Nabenve bananiwuza machitdwe yake yamushe nakuchita lipoti mawu yanga kuli yenvee. Nkalata zinatumiwa kuli ine kuchokela kuli Yobiya kuti aniyofye.