1 Ndipo bantu na bakazi banyamu kulila kwachikulu mosusana ba Yuda bazawo. 2 Chifukwa kunali benangu banali kukamba kuti, "Na bana batu bamuna naba kai tili bambili. Tiyeni titenge tirigu kuti tidye nakunkala wa moyo." 3 Kunali benangu nafuti bana kamba kuti, "Tikongolesa minda yatu, mind yampesa, na manyumba yatu kuti titenge tirigu muntawi yanjala." 4 Benangu banakamba kuti nafuti, "Takongola ndalama kulipila musonko wanfumu pa minda yau na minda yampasa. 5 Koma manje tupi latu na gaz niyimozi naya abal batu, ndipo bana batu nibamozi bawo. Takakamizidwa kugulisa bana batu bamuna naba kazi kunkala bakapolo. Bana batu bakazi benangu niba kapolo kudala. Koma sizili mumpavu zatu kutandiza chifukwa bamuna benangu manje bali na minda zampesa yatu." 6 Ninakalipa pamene ninavela kulila kwawo na mawu aya. 7 Ndipo ninaganiza pal ichi, naku chita upilo wampavu kuli bolemekezeka nabo yanganila. Ninakamba kuti kuli benve, "mufuna chiwongola zanja, aliyense kuchokela kuli bale wake 8 nakumba kuli benve, "Kuli ise, tili nazo. kulinga na mpamvu zatu, tinagwa nafuti kuchokela ku ukapolo able atu ba Yuda bamene benze bana gulisiwa ku chalo, koma munagulisa able banu chakuti bagulisiwe kuli ise!" bankale chete ndipo sibanapezekenamawo yo kamba. 9 Naafuti ninakamba, "Vamene muchita sivabwino. Simuyenda kuyenda mukuyopa Mulungu watu kupwea bonyoza bamu chalo bamene bali niba dani batu? 10 Ine na abale banga na kapolo banga tibakongolesa ndalama na tiligu. Koma tifunika kusiya kulipilisa chiwongola zanja pa nkongole izi. 11 Bwezani kuli benve lelo yamene minda yawo, minda yampesa, munda wa azitona, manyumba yabwo na kuchuluka kwa ndalama, tiligu, vinyu yasopano namafut yamene munafuna kuli benve." 12 Ndipo banakamba kuti, "Tizabweza zamene tinatenga kuli benve, sitizafuna nachilichonse kuchokela kuli benve. Tizachita zamene watiwuza." Ndipo ninayitana ansembe, naku balumbilisa kuti bachite zamerne bana lonjeza. 13 Nina nyan'anyisa mwnjiro yanga nakukamba kuti, "Mulungu anayang'nyise kuchokela munyumba mwake na katundu ya muntu aliyense wamene sazasunga lonjezo yake. Chakuti anyang'nyisiwe naku kesedwa." Bonse bolongana banakamba kuti, "Ameni," Ndipo banatamanda Yehova ndip bantu banachita zamene bana lonjeza. 14 Kochokela ntawi yamene ninansankiwa kunkala kazembe wabo mualo ya Yuda, kuchokela mumwaka wa twenti kufikila mumwaka wa sate-tu wa Artaxerxes mfumu, myika twelufu, ngakale ine kapena abale banga chokudya chopasiwa kuli kazembe. 15 Koma bakazmbe bakale banaliko banayika zolemesa zikulu pa bantu, nakutnga kuli benve masekeli ya siliva ya fote kuckela kuli zokudya zawo na vinyu. nabakapolo babo banali mfumu pa b antu. Koma sinachite ivi chifukwa chakuyopa Mulungu. 16 Naine ninakonkaya kusebenza pachibumba, ndipo sitina gila malo, ndipo bonse bakapolo banga banankala pamozi pa nchito. 17 Pa tebulo yanga kunali ba Yuda yangila bawo, bamuna bali 150, kuchosela baja banabwela kuli ise kuchokela mukati mwachalio chenzo tizignuluka. 18 Manje zamene zenza pangiwa masiku yonse inali ng'om e imozi, nkosa zili sikisi, na zinyoni, mumasiku yonse yali teni mitundu yonse ya vinyu inali yambali, koma kuli ivi vonse sinina oindeko gawo lazakudya kuli kazembe, chifukwa nchito inali yolema pa bantu. 19 Nitaneni munzelu, Mulungu wanga, bali zabwino, chifukwa chazamene nachitlia bantu aba.