1 Aba ndiye ba sembe na Alevi ana bwela na Zerubabeli mwana wa SHeatili na Yesuwa: Seraya, Yeremeiya, Ezira, 2 Amariya, Malluki, Hattusi, 3 Shicaniya, Rehumi, na Meremoti. 4 Aba banali Iddo, Ginnetoni, Abija, 5 Mijamini, Moadiya, Bilga, 6 Shemaiya, na Joiaribu, Yedaiya, 7 Sallu, Amoki, Hilkiya, na Yedaiya, aba ndiy anali Azisogoleli baba kulu ba sembe na bosebenza nabo mu masiku ya Yesuwa. 8 Alevi anali Yesuwa, Bunni, Kadmieli, Sherebiya, Yuda, na Mattanya, anali kuyanganila nyimbo zo yamikila, pamozi nabotandizila. 9 Bakbukiya na Unni, botanduza nabo, bana imilkla pa sogolo pabo ntawu yo sonkana. 10 Yeshuwa anali ni tate wa Yoiakimu, Yoiakimu anali tate wa Elisibu, Elishibu anali tate wa Yoiada, 11 Yoiada anali tate wa Yonathani, na Yonatani anali tate wa Yaddwa. 12 Mu masiku ya Joakimu aba banali ba nsembe, sogoleli ama banja: Meraiya musogoleli wa Seraiya, Hananiya anali musogolei wa Yeremiya, 13 Meshullamu anali musogoleli wa Ezira, 14 Yehonani anali musogolei wa Amariah, Jonathani anali musogolei wa Malluki, na Yosefe anali musogoleli wa Shebaniya, ***kumasulila kwa manje ali Malluki ngati kuluga misa Malluki muchilembedwevcha Heberi, kumasulila ko ona kwazina iyi ponekela mu Nehemiya 12;2.*** 15 Adna anali musogoleli wa Harimu, Helkai musogoleli wa Mereoti, 16 Zakariya anali musogoleli wa iddo, Meshullamu anali musogoleli wa Ginnetoni, na 17 Zichri anali musogoleli wa Abija; Piltai anali musogoleli wa Miniamini na Moadiya, 18 Shammuwa anali musogoleli wa Biga, Yehonatani anali musogleli wa Shemiya, 19 Mattenai anali musogoleli wa Yoiaribu, Uzzi anali musogoleli wa Yedaiya, 20 Kallai anali musogolei wa Sallu, Eberi anali musogoleli wa Amoki. 21 Hashabiya anali musogoleli wa Hilkiya, na Netaneli anali musogoleli wa Yedaiya. 22 Mu masiku ya Elisabu, mu Levi Elisha, Yoida, Yohanani, na Yaddwa anali analembdwa ngati oyanganila ma banja, naba nsembe ana lembedwa eja tawi ulamulilo wa Dariyasi mu Fasini. 23 Bobadwa mumbuyo wa Levi, azi sogoleli ama banja yabo anali bana lembedwa muma buku yosungilamo kufikila masiku ya Yohona ni mwana wa Elishibu. 24 Azisogoleli waba Levi anali Hashabiaya, SHerebiya, na Yeshuwa mwana wa Kadmeli, na bottandizila, ana imilila kusogolo kwabo benve ku peleka ma tamando naku yamikila, kuyanka bali na bali, monvelela malamulo ya Davidi, kapolo wa Mulungu. 25 Mattaniya, Bakbukiya, Obadiya, Meshullamu, Talmon, na Akkubu anali osunga viseko kuimilila kulonda kosungila vintu pa chiseko. 26 Anatumikila mu masiku ya Joikimu mwana wa Yeshuwa mwa wa Yozadaki, namu masiku ya Nehemiya kazembe ndipo kwa Ezira wa sembe ndi kalembela. 27 Pasiku yoika chipupa cha Yelusalemu, bantu anasakila kuli konse benze ku nkala, ku baleta ku Yelusalemu ku sangala kukkiza mwa chisangalalo, ndi zoyamikila na kuimba na mitololo, luti, na zoimbila. 28 Ku sokana kwabo imba bwela pamuzi mu muzinda ozungulila Yelusalemu namu minzi zaba Netofatite. 29 Ndiponso ana chokeka kuli Beti Gigali naku minda kwa Geba na Azmaveti, ndaba oyimba anazimangila beka minzi zabo ku zungulila Yerusalemu. 30 Asembe na Alevi anazi yesesa benve beka, ndipo bana yelesaso bantu, polbea chiseko, na chipupa. 31 Ndipo ninali na azisogoleli ba Yuda ku yenda pa mwamba ya chipupa, ndipo nina sanka magulu ya bili oyimba anapeleka matamando, imozi ina ku zanja la manja ku yenda kalobela chiseko cha Dungi 32 Hoshaiya na pakati patula azisogoleli ba Yuda anaba konka benve, 33 ndipo pambuyo pabo pana yrnda Azariya, Ezira, Meshullamu, 34 Yuda, Benjamini, Shemaiya, Yeremiya, 35 ndipo asembe bena bana bamuna na malupenga, na Zakariya mwana wa Jonatani mwana wa SHemaiya mwana wa Mattaniya mwana wa Micaya mwana wa Zaccuri mwana wa Asafu. 36 Kuja futi kunali abulu ba Zakariya, Shemaya, Azareli, Milalai, Gilali, maai, Netaneli, Yuda, Hanani, nazoimbilako za Davidi kapolo wa Mulungu. Ezira kalembela anali pa sogolo pabo benve. 37 Pasogolo pa chiseko ana yenda pa mwamba pa manela pa muzinda wa Davidi, pokwelela ma nela ku chipupa pa mwamba pa nyumba ya Davidi, ku chiseko cha manzi kumu mawa. 38 Oyim a bena amene anapeleka matamand ana endaso bali ina, nina ba konka abenve pa chipupa na gulu pakati ya bantu, pamwanba poonelako pa ovensi, k chipupa chotabalala, 39 na pamwamba pa chiseko cha Efuremu, na ku chiseo chakudala, naku chiseko cha somba na poyanganila pa mwamba pa Hananeli na po yanganila kuminama kumi, ku chiseko cha belele, ndipo pana imilila pa chiseko cha malonda. 40 Ndipo bonse bama imbidwe bamene anapeleka maamiko anatenga bali yambo mu nyumba ya Mulungu, ndipo nina tengaso bali yanga na pakati yaba kazembe na ine, 41 ndipo ansembe anatenga malo: Eliakimu, Maaseya, Miniamini, Mikaya, Elioenai, Zakariya, na Hananiya, nama lupenga. 42 ndiponso Maaseiya, SHemaiya, Eleazari, Uzzi, Yehohanani, Malkija, Elamu, na Ezira, naba imbidwe anazi panga azisogoleli benve na Yezrahiya anali musogoleli wabo. 43 Anapeleka nsembe yaikulu eja siku, naku saugalala, ndaba Mulungu analengesa benve kusangalala nachi sangalalo cha chikulu, ndiponso Azimai na bana banakodwela. Ndipo chisangalalo cha Yerusalemu kunveka kutali. 44 Pa siku ija amuna bana sankiwa ku yanganila ko sungila zitu zo souka, zoyamba kupya zamu munda, na cha kumi, ku sokansia bali yo enela palamulo yaba samba na kwa Alevi, aliyense ana igabiliwa ku senza mu munda pafupi na minzinda. Kamba Yuda anasangalala pali ba nsembe na Alevi ana imilila pa sogolo pabo benve. 45 Ana chita nchito ya Mulungu wabno, na nchito yo yelesa, ndipo sa ana chitaso amimbidwe na bosunga viseko, muku sunga malamulo ya Davidi ndipo ya Solomoni mwana wake mwamuna. 46 Kuchokela ku dala, mu masiku ya Davidi na Asafu, kuna ku sogolewa kuli boyimba, ndipo kunali nyimbo zama tamando na kuyamikila kuli Mulungu. 47 Mu masiku ya Zerubabeli ana peleka bali yofunikila kuli boyimba nabo sunga viseko. Ana sunga kuba zo yelesedwa bali yabo yamene ina ya Alevi, ndipo Alevi ana ika kumbali zoyelesedwa bali yabo badwa mumbuyo mw Aaroni.