Mutu 13

1 Pa siku ija bana belenga mu buku ya Mose mukunvela kwa bantu. Zina lembedwa kutu kulebe mu Amoni mwina Mohabati kuti safunika ku bwala muku sonkana na Mulungu muyayaya. 2 Ichi chinali chifukwa kamba bana bwela kuli Isilayeli. Nga nkale choncho, Mulungu watu ana pindamula tembelelo ku nkala daliso. 3 Pamene anavela malamulo, banazi patula benve kuli ba Isilayeli aliyense wa chilendo muntu. 4 Manje sana chite izi Eliashabu wa nsembe ana sankiwa oyanganila zosungilamo zintu mu nyumba ya Mulungu watu. Anali wa chibululu wa Tobiya. 5 Eliashabu anamu kozeka Tobiya mosungila mukulu, mwamene pa chiyambi anali ku sungila chaulele cha beu, zonukila, makatundu na chakumi cha beu , lamuliliwa ku nkala ya Alevi, boyimba, osunga viseko, nazo sonka kuli ba kulu ba sembe. 6 Koma mutawi iye chinali ku Yelusalemu. Kamba mu chaka cha ma kui yatatu na zibili ya Artazekisi mfumu yaku babulo nina yenda kuli mfumu. panapita ka ntawi nina pempa mupata kuli mfumu ku yenda, 7 ndipo bwelela ku Yelusalemu. nina nsesesa kuipa mutima wa Eliasabu anachita paku pasa Tobiya musungilamo zintu mu nyumba ya Mulungu. 8 Ichi chinali chosa kondwelesa kwa ine nia taya zonse zamu nyumba ya Tobiyasi makatundu ku chosa mu sunila,o vintu. 9 Nina lamulila kuti ayeleswele mo sungila mo vintu, ndipo nina bwezalamo zintu za mu nyumba ya Mulungu, benuo ya cha ulele, nazo nunkililsa. 10 Nina bwela kuziba kuti Alevi bali yabo siba na pasiwe kuli benve, ndiponso banali banataba, aliyense ku munda wake, Alevi nabo imba bamene analu kusebenza. 11 Ndipo ninan vikila akulu naku kamba kuti "chifukwa chani nyumba ya Mulungu yalekelelwa?" Nina baleta pa mozi nakubaika pa malo yabo. 12 Ndipo onse Ayuda analeta chakumi cha beuo, vinyu chasopano, na mafuta ku nyumba sungila vintu. 13 Nina sanka ngati asunga pa nyumba yo sunhilamo vintu Shelemiya wa ansembe na Zadoki kalembela, naku chokela kwa levi. Pedaya, onkankapo kwa benve anali Hanai mwana wa Zaccuri mwana wa Mattaniya, ndaba anali bobelengeka okulupilika. Zi nchtio zabo kunali kupeleka zofunikila kuli azitandizi babo. 14 Nikubuseni ma ganizo, Mulungu wanga, kumbali iye, ndipo musa chosepo za bwino zamene na chita mu nyumba yamu Mulungu wanga nazi chinto zonse. 15 Mu masiku yaja nina mu Yuda bantu ali ku gulisa vinu pa Sabata na kubwela ku unjika mbeu naku ika bama bulu, ndipo na vinyu, pesa, mukuyu, na zosiya zolema ma katundu. Yamene bana leta mu Yelusalemu pasiku ya Sabata, nina ba chenchenza ku kulisa vikudiya pa siku ija. 16 Amuna aku Taya anali ku nkala mu Yelusalemu anali ku leta saomba na makatundu yosiyana siyana, ndipo anali ku gulisa pa Sabata ku bantu baku Yuda na mu muzinda! 17 Ndipo ina ba konkela bolemekzedwa, mu Yuda, "Nanga ni chani zoipa zamene mu chita izi, kulakwila siku la Sabata? 18 kodi ba tate sibana chite zamene izi? Kodi Mulungu sana tiletele zoipa zonse paise pa muzinda? manje muleta kukwiya pa Isilayeli kamba ko lakwila Sabata." 19 Pamene kuna fipa pa chiseko cha Yelusalemu isana fike Sabata, nina lamulila kuti viseko valiwe kuti siya funika ku segulewa kufikila ika pa Sabata. nina ika ba chinto banga benangu pa chiseko kuona kuti basa bwelesa makatundu mukati pa siku la Sabata. 20 Ama chita malonda benve na gulisa yosiyana siyana zovala mumakapu pajapa Yerusalemu kamozi mwina kabili. 21 Koma nina ba chenchenza benve, "Chifukwa chani mu sokana paja pa chipupa? ngati muza chit futi, niza ku menyani na manja yanga! "kuchokela ntawi ija bana leka ku bwela pa Sabata. 22 Ndipo nina lamulila Alevi kuzi yelesa beka, naku bwela naku londa viseko, yeselsa siku ya Sabata. Nikubu seni maganizo kwa icho futi, Mulungu wanga, ni chitileni chifundo ine chikwa kamba ka chipangano mozipela yamene muli nayo kuli ine. 23 Mu masiku yaja naineso nina oa ma Yuda bamene bana kwatila bakazi baku Asrdodi Amoni, na Mohabu. 24 Pakati pa bana babo banali luziba ku kamba chitundu cha chi Yuda, koma kambe chitundu cha bantu bena. 25 Nina fikila benve, naku batembelela benve, naku ba menya benango naku ba donsa matu yabo benve. Ninaba lengesa kulapila kuli Mulungu, Kukamba kuti, "Musa pase bana bakazi kuli bana babo mwina kutenga bana babo bakazi kupasa bana bamuna. Mwina kwa imwe benve. 26 Kodi Solomoni mfumu ya Isilayeli ana chimwa kamba kabazi mai? Ngale maiko yena kuna libe mfumu monga enve, Ndipo Mulungu anamupanga enve mfumu wa Isilayelii onse. nga nkale choncho, akazi bake bachilendo bana mu lengeza iye ku chimwa. 27 Kodi ise tinvelele kwa iwe naku chita zoipa za zikulu, naku chita mosa kulupililika kwa Mulungu watu oaku kwatila azimai ba chilendo?" 28 Umozi mwana mwamuna wa Yoida mwana wa Eliashibu mukuli wa nsembe anali mupongozi wa sanibalati mu Horoneti. kwaicho nia lengesa enve ku taba kuchoka pa manso yanga. 29 Nikumbuseni maganizo, Mulungu wanga, chifukwa ba sokoneza mukulu wa nsembe wabo, ndipo chipangano chaba nsembe na a levi. 30 kwaicho nina ba yelesa benve ku choa kuli va chilendo, naku khazikisa zi nchtio za a nsmebe na Levi, aleyemse kuku nchito yo pasiwa. 31 Ninapeleka kumi zopeleka chaulele pa ntawi yo sankiwa nazo yamba kupiya mu munda. Nikumbuseni maganizo, Mulungu wanga, kuno bwino.