Mutu 11

1 Azisogoleli ba bantu bana nkala mu Yelusalemu, ndipo bantu bonse bana chita mayele kuleta umoze pali bali kumi ku nkala mu Yelusalemu, Muzinda oyela, ndipo sanu ndi anai banasala mu muzinda zina. 2 Ndipo bantu bana dalisa bonse banazipeleka ku nkala mu Yelusalemu. 3 Aba ndiye akazembe bamu muzinda bamene bana nkala mu Yelusalemu. ngale choncho, mu muzinda wa Yuda aliyense ana nkala mu malo yabo kuikilako benango ma Isilayeli, Asembe, Alevi, osebenza mu nyumba ya Mulungu, na bana bobadwa mumbuyo mwa Solomoni ba nchito bake. 4 Mu Yelualemu muna nkala bena bobadwa mumbuyo ba Yuda na bena bobadwa mumbuyo ba Benjaameni. Bantu baku Yuda kuikilako: Athaiya mwana wa Uzziya mwana wa Zakariya mwana wa Amariya mwana wa Shefatiya mwana wa Mahalaleo, Obadwa mumbuyo mwa Perezi. 5 Kunali Maaseiya mwana wa Beruchi mwana wa Kal-Hozeh mwana wa Hazaziya mwana wa Adaiya mwana wa Joiaribu mwana wa Zachariya, obadwa mumbuyo mwa Shela. 6 Bonse bo badea mumbuyo mwa Perezi ana nkala anali 468. Anali amuna bo imilila. 7 Aba ndiye bobadwa mumbuyo mwa Benjamani: Sallu Meshullamu mwana wa Meshullamu mwana wa Yoedi mwana wa Fedaiya mwana wa Koliya mwana wa Maasiya mwana wa Itho mwana wa Yeshaiya, 8 ndipo b mu konka enve, Gabbai na Sallai, 928 Amuna. ***osati baja bomu konka enve bena bopunzila chiganizo chao abale bake chifukwa kamba kama magidwe yana onekela kuli Nehemiya 11;13, 14, 17, na 19.*** 9 Yowili mwana wa Zichri anali obayanganila na Yuda mwana wa Hassenuya anali woi chibili mu lamulilo pa muzinda. 10 Ku chokela kwa ba sembe: Yedaiya mwana wa Yoiribu, Yakini, 11 Seraiya mwana wa Hakiya mwana wa Meshullamu mwana wa Zadoki mwana wa Meraioti mwana wa Ahitubu, Mukulu wamu nyumba ya Mulungu, 12 nabo tandizila amene ana zebeza mu nyumba, 822 amuna, pamozi na adaiya mwana wa Amzi mwana wa Zakaliya mwana wa Pashuri mwana wa Malkija. 13 Abale bake banali oyanganila mutundu, 242 amuna: na Amashsai mwana w Azareli mwana wa Ahzai mwa wa Meshilemoti mwana wa Immeri, 14 ndi abale bake, 128 asilikali omenya nkondo: oba yanganila wabo Zabdili mwana wa Haggedolimu. 15 Ku chokela kwa Alevi: Shemaiya mwana wa Hasshubu mwana wa Azrikamu mwana wa Hashabiya mwana wa Bunni, 16 na Shabbetai na Yozabadi, anali kwa izi sogoleli kwa Alevi ndipo ana yanganila nchito yopanja ku nyumba ya Mulungu. 17 Kunali Mattaniya mwana wa Mika mwana wa Zabdi, obadwa mumbuyo mwa Asafu, wamene ana sogolela ana yaba ma pempelo yoyamikila, na Bakbukiya, wa chibili pakati pa abale bake, na Abda mwana wa Shammuwa mwana wa Galali mwana wa Yedutuni. 18 Bonse Alevi mu muzinda oyela kebelnga 284. 19 Osunga veseko: Akkubu, Talmonu, naba bale babo, analonda veseko volobelako, 172 amuna. 20 Osalapo ba Isialyeli ba sembe na Alevi banali mu muzinda za Yuda. Aliyense ana nkala mu malo yake yolobelela katundu wake. 21 Osebenzela mu nyumba ya Mulungu ana nkala mu ofeli, na zina na Gishaoa anaba yanganila benve. 22 Akulu oyanganila Alevi mu Yelusakemu anali Uzzi mwana wa Bani mwana wa Hasabiya mwana w Mattaniya mwana wa Mika, obadwa mumbuyo mwa Asafu, amaimbidwe pa ncgito yamu nyumba ya Mulungu. 23 Banali paulamulilo kuchokela kwa mfumu, na monenesa ulamulilo una paswa kuli bamu imbidwe masiku yonse yofunikila. 24 Ndipo Petahiya mwana wa Meshizabeli, obadwa mumbuyo mwa Zera mwana wa Yuda, anali kumbali ya mfumu mu kani zokuza bantu. 25 Ku bwela ku minzi na minda zabo, bantu bena baku Yuda ana nkala mu Kiriati Arba na minzi zabo, ndipo mu Diboni na minzi zake, namu Yekabuzeli na minzi zake, 26 na mu Yesuwa, Molada, Beti Peleti, 27 Hazari Shuali, and na Beersheba na minzi zake. 28 Bantu bena bamu Yuda ana nkala mu zigilagi, Mekona na minzi zake, 29 Enrimmoni, Zora, Jarimuti, 30 Zanoa, Adullamu, na minzi zake, na mu Lachisi minsa zake na Azeka na minzi zabo. Choncho ana sokana kuchokela ku Beersheba kukila mu musipu wa Hinnomi. 31 Bobadwa mumbuyo mwa Benjamite mu Geba, Mikmashi, Aija, Beteli na minzi zake, 32 Anatoti, Nobu, Ananiya, 33 Hazon, Rama, Gittaimu, 34 Hadidi, Zeboimi, Neballati, 35 Lodi, na Ono, musimpu wabo sema. 36 Alevi bena ana nkala mu Yuda ana oelela bantu baku Benjamini.