Mutu 3

1 Manje Mose anali akali kubusa vobeta va Yotero mu pongozi wake, wansembe wa Midiyan. Mose anasogolela vobeta ku mbali. yakutali ya chipululu anafika pa Horebu, lupili Mulugnu. 2 Kwamene uko Mungelo wa Yehova anaonekela kuli enve muchi mbili-mbili chamulilo musanga. Mose anayangana, ndipo onani, musanga unali kubuka, koma chisamba sichenze kunyeka. 3 Mose anakamba, "nizapatukila kumambali kuti ni one ichinchintu chodabwisa, chifukwa ni chani chisamba sichinyeka." 4 Pamene Yehova anaona kuti anapatulila pa mbali kuyangana, Mulungu anamuitana kuchokela muchisamba na kukamba, "Mose, Mose." Mose anakamba kuti, "nili pano." 5 Mulungu anakamba kuti, "osabwela pafupi! Vula nsapato zako ku mapzai yako, Chifukwa pamalo apa pamene waimilia ni popatulika kuli ine." 6 Anaikapo, "Ndine Mulungu wa batate bako, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki, na Mulungu wa Yakobo." Pamene apo Mose anazivininkila ku menso, chifukwa anayopa Mulungu kuyangana Mulungu. 7 Yehova anakamba, "Naona zo'ona kuvutika kwa bantu banga bali mu Iguputo, namvela kulila kwao chifukwa chabantu bobasebenzesa, chifukwa zakutika kwao. 8 Naseluka pasni kuba masula kuchokela ku mpavu zama Iguputi na kubaleta mumalo ya bwino, malo yakulu, kuziko ya mukaka na uchi ku malo yaku kanani, Ahiti, Aamol, Aperz, Aperizi, Ahivi na Ayebusi. 9 Manje kulila kwa bana banga kwafika kuli ine, ndiponso, naona kutiiliziwa kwawelesawa nama Iguputo. 10 Manje apa, Nizakutuma kuli Farao kuti ubwelese bantu banga, ba Isilayeli, kubachosa mu Iguputo." 11 Koma anakamba kuli Mulungu, "Ndine ndani ine, kuti niyende kuli Farao naku bwelesa bana ba Isilayeli kubachosa mu Iguputo?" 12 Mulungu anayanka, nizamkala naiwe nditu. Ihci ndiye chamene uzabilako kuti ine nakutuma. vikachosa bantu mu Iguputo, uzaniyamika in pa lupili ino." 13 Mose anakamba kuli Mulungu, "Pamene nizayenda kuli ma Isilayeli na kubauza. Mulungu wa makapolo anituma kuli imwe,' ndipo baka kamba kuli ine, zina yake nindani? nichani chamene nizakamba? 14 Mulungu anakamba kuli Mose, "INE NDINE MWAMENE NDILILI." Mulungu anakamba, ufunuka kukamba kuli ba Isilayeli, INE NDINE anituma kuli iwe. 15 Mulungu anakambanso kuli Mose ufunika kukamba ku Isilayeli, 'Yehova, Mulungu wamakolo yanu, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki ndi Mulungu wa Yakobo, anituma kuli iiwe. Iyi ndiye zina kumbukiliwa na mibadwo yonse. 16 Yenda ulongane bakuluvbonse bamu Isilayeli pamozi. Kamba nabo kuti, Yehova, Mulungu wa makolo, , Mulungu wa Abrahamu, Isaki ndi Yakobo, aonekela kwaine naku kamba, "nankala ninyang'ana ndipo naona vamene vachitika kuli imwwe mu Iguputo. 17 Nalonjeza kukuchosani mumalo ya botitiliza mu Iguputo kukupelekani kumalo yaku kanakni, Ahiti, Aamori, Aperizi, Ahivi na Ayebusi, muziko yoyendamo mukaka na uchi." 18 Bazakumvelelani imwe. Iwe na bakulu bamu Iguputo, ndipo mufunika ku mu'uza, .Yehova, Mulungu wa Aheberi, akumana naise. Manje tiyende uledno wa masiku yatatu muchipululu, kuti tikapeleke nsembe kuli Yehova Mulungu watu. 19 Koma niziba mfumu yaku Iguptuo sizakuleka ni kuti muyende, koma chabe kukakamiza kwanja yake. 20 Nizatambasula kwanja yanga na kumenya ma Iguputo navo dabwisana vonse pake azakulekani. 21 Nizapasa aba bantu mwai pamenso yama Iguputo, chakuti mukachoka , simuzayenda mulibe chili chonse. 22 Muzimai alionse azafunsa siliva na golide vokomesela vovalika kuchoka kuli bantu bake bamu Iguptuo na bazimai bankala mu manyumba yapafupi. muzavi ika pali bana banu bamuna na bakazi, munjila yiy muza ononga ma Iguputo."