Mutu 2

1 Manje mwamuna wamutundu wachi Levi anakwatila mukazi wachi Levi. 2 Mukazi anakala namimba naku bala mwana mwamuna. Pamene anaona kuti anali mwana mwaumoyo wabwino, anamubisa myezi itatu. 3 Koma pamene analeka kumu bisa kumubisa, anatenga basiketi ya papiras, naku mata na bituman na ulimbo. Manje anamufakomo mwana mukati nakufaka pama tete mumanzi. 4 Mulongo waka anaimilila patali kuti aone vizachitika kuli enve. 5 Mwana mukazi wa Farao anabwela kusamba kumanzi apmene bosebenza bake benze kuyenda mumbali mwa manzi, anaona basiketi pakati pa tete naku tuma banchtio bake baitenge. 6 Pamene anaisegula, anaona mwana. Onani, mwana anali kulila. anankal nachifundo pali enve naku kamba, "Uyu zo'ona nimwana waumozi wama Heberi." 7 Koma mulongo waka mwana anuza mwana wa Farao, "kodi niyende kusakila mukazi wachi Heeri wamene azayamba kusunga mwaa uyu?" 8 Mwana mukzai wa Farao abaumza iye, "Yenda." naku kamusikana kangono kanayenda nakutenga bamai bake ba mwana. 9 Mwana mukazi wa Farao anauza bamai ba mwan, Tenga mwana uyu uninyosheleko, ine nizakulipila." Pamene mukazi anamutenga naku munyosha. 10 Pamene mwana anakulako, bana muleta kuli mwana mukazi wa Farao, anso anankala mwana wake. Amamupasa zina ya Mose naku kamba, "chifukwa ninamu chosa mu manzi." 11 Pamene Mose anakula, anayenda kunja kubantu bake anaona kusebenza maingi kwao. Anaona mu Iguputo anmenya bantu bake. 12 Analangana uku kumbali na uku kumbal, koma pamene anaona kuti kunalibe aliyense, Anapaya mu Iguputo naku bisa tupi yake mu michenga. 13 Anachoka siku yokankapo, na, onani, bamuna babili ba chi Heberi benze kumenyana. Anauza umzi wamne enze olakwa, "Nichani chamene umenyala muzako?" 14 Koma mwamuna anamu'uza, "nindani akupanga mukulu na otiweluza pali ise? Nanga uganiza kunipaya ine monga mwamene unaoaila mu Iguotuo?" Pamene apo Mose anankala na manta anakamba, " vamene nina chichita zo'ona vazibika kuli benangu." 15 Koma pamene Farao anavela pali ichi, anayesa kupaya Mose. Koma anamutaba Farao naku nkala ku ziko yaku Midani. Kuja anakankala pansi pa mbali ya chisime. 16 Manje wansembe waku Midani anali nabana bakazi bali seveni. Bana bwela, kutapa manzi, nakmunfaka muvotapila manza kuti bamwese nyama zosunga. 17 Bobetela bana bwela naku yesa kuba pisha, koma Mose anayenda naku batandiza. Pamene apo anaba mwesela nyama zosunga. 18 Pamene basikanaka banayenda kuli Reueli atate bao, anakamba, "nichani mwabwela kunyunmba musanga lelo?" 19 Bana kamba, " waku Igiuputo atipulumusa ise kuli mbusa. Ati tapilana manzi naku mwesa nyama zosunga." 20 Anabauza bana baka bakazi. "Nanga alikuti? nichani mwamusiya mwamuna? Muitaneni kuti adye chakudya naise." 21 Mose anavomela kunkala na mwamuna, wamne futi anamupasa Zipora mwana wake mukazi kuti akwatile. 22 Anabala mwana mwamuna, na Mose anamupasa zina Geshomu, yachilendo." 23 Pamene kunapita ntau, mfumu yaku Iguputo inafa. Ba Isilayeli banalila chifukwa chanchito yaukapolo. Bana lila kufuna tandizo, naku pempa kwao kunayenda kuli Mulungu chifukwa chaukapolo. 24 Pamene Mulungu ananvela kulila kwao, Mulungu anakumbukila pangano yamene inali pakati pa enve na Abrahamu, Na Isaki, na Yakobo. 25 Mulungu anabaona bana ba Isilayeli, naku ziba kuvutika kwabo.