Mutu 1

1 Nyimbo ya Nyimbo, yamene ni ya Solomoni. 2 Ha, Mwakuti agani fiyofiyote ine naku fiyofiyotewa na pakamwa pake, 3 Mafuta yanu yozoza yonunkhila bwino; zina yako ni mafuta onunkhila bwino, chifukwa chake asikana amakukonda iwe. 4 Nditenge muyende naine ,Andipo tiza taba. 5 Ndine ofipa koma wokondewa, ana akazi imwe a ku Yerusalemu; ofipa ngati mahema ya Kedara, okongola ngati nsalu za Solomoni. 6 Musaniyang'ane chifukwa ndine ofipa, chifukwa zuba ya shoka ine. Bana wa amai bamuna bana kalipa naine; Banani ika oyang'anila minda yamphesa, koma sininasunge munda wanga wamphesa. 7 Niuze, iwe wamene mutima wanga ukonda, udyesela zibeto zako kuti? Umapumulisa kuti zibeto zako ntawi yamuzuba? Nisanduka bwanji muntu oyendayenda na gulu ya abale bako? 8 Ngati suziba ,okongola kwambili pakhati pali bakazi bonse, kokani njila ya nkosa zanga, ndipo dyeselani bana banu ba mbuzi pafupi na mahema yamu busa. 9 Okondewa wanga, nikulinganiza na mwana mkazi pakati pa magaleta ya Farao. 10 Mbovu zako ni zabwino na zokongolesa, mukhosi wako na tambo za meyala yokongola mumukosi. 11 Tikupangila zokongolesela zagolide na zomangila zasiliva. 12 Mfumu ili gone pabedi pake, nade wanga anali kuchosa kununkila kwake. 13 Okondewa wanga alimonga tumba ya mule yamene imagona pakati pa mabele yanga. 14 Okondewa wanga ali ngati kuli ine sango Ya maluba ya heni mumuda yamphesa ya En-Gedi. 15 Nvela ,ndiwe okongola, okondewa wanga; nvela, ndiwe okongola; menso yako yali kwati nkunda. 16 Mvela, ndiwe okongola, okondedwa wanga, ndiwe okongola bwanji. Zomela zobilibila na kama yatu. 17 Mupanda wa nyumba yatu ni mukungudza; Mitengo yatu ni yabwino.