Mutu 134

1 Nyimbo yokwela. Bwelani, lemekezani Yehova, iwe bonse atumiki ya Yehova, imwe bamene mukutumikila usiku munyumba ya Yehova. 2 nyamulani manja yanu kumalo yoyela ndipo lemekezani Yehova. 3 Yehova akudaliseni kuchokela ku Ziyoni, wamene analenga kumwamba na ziko yapansi.