Mutu 134
1
Nyimbo yokwela. Bwelani, lemekezani Yehova, iwe bonse atumiki ya Yehova, imwe bamene mukutumikila usiku munyumba ya Yehova.
2
nyamulani manja yanu kumalo yoyela ndipo lemekezani Yehova.
3
Yehova akudaliseni kuchokela ku Ziyoni, wamene analenga kumwamba na ziko yapansi.