1 “Kawirikawiri bankala boniukila kuchokela kubwana wanga,” leka Isiraeli ikambe . 2 Ntawi zambili bama nkala boniukila kuyambila kuubwana wanga, koma sibananigojeze. 3 Bolima balima pamusana panga;banatalimpisa mizela zawo. 4 Yehova ndiye wolungama; adula ntambo za oipa.” 5 Bachitisiwa manyazi na kubwelela kumbuyo, bamene bazondaZiyoni. 6 Bankale monga mauzu yapakomo yamene yamafota yakalibe kukula 7 yamene siyanga pake mumanja mwa okolola kapena m’bokosi ya omanga mbewu. 8 Bamene bapitapo basa kambe kuti, “Madalitso ya Yehova yankale pali imwe, tikudalisani muzina ya Yehova.