Mutu 10

1 Soka kuli aba bamene baika malamulo yosalunama naku kamba zosalungama na zilemba. 2 Anapoka chilungamo kuli losauka, kubela ovutika banty ufulu wabo kutengela akazi ofedwa bamuna, kutenga balibe makolo babo kunkala monga vinyama. 3 Uzachita chani pasiku ya chiweluzo pamene chionongeka chizabwela kuchokela kutali? nikuli ndani kwamene uzatabila kufuna tandizo, ndipo muzasiyila ndani chuma? 4 Palibe chizasala, ndipo uzankala pakati pabo mangiwa na kupezeka pabo paiwa, muli ivi vonse, ukali wake suseluka, mwakuti kwanja kwake nikotambuluka. 5 soka kwa Asilkya, nkolo yawukali wanga, ndodo yamene nizawonesera ukali wanga! 6 Nizamutuma enve kuziko yozikuza ndipo kusuana nabantu bamen anyemula kuzuli;a kwaukali wanga. Ninamulamulila enve kutenga zopoka, kubagwita, ndipo nakubadyaka benve ngati matika mumuseu. 7 Koma sizamene enze kufuna, mwina saganizila munjila iyi. Nimumutima nakuchosapo ma iko yambili. 8 Akamba kuti, "Bana obadwa kuma mfumu kodi si mfumu? 9 Kodi kalino salimonga kachemisi? Kodi Hamati ali monga Apadi? kodi samaliya sali monga Damasika? 10 Kwanja kwanga kwaogonjesa maufumo amafano, zosema zawo zenze zopambana zamu Yelusalemu na samaliya, 11 mwamene ninachita kuli Samaliya nama fano yake yopanda pake, sinizachita chimozi ku Yelusalemu namilungu yake yopanga?" 12 Pamene Ambuye akusiliza nchito yake palupili la Zayoni naku Yelusalemu, nialanga malankulidwe ozikweza mutima wa mfumu ya Asiliya nakuyangana kwake kozi kweza. 13 Akamba kuti. "Mumpamvu zanga namunzelu zanga nina chita. Nilinako kumvesesa, nansopano malile wa bantu, Naba bela chuma chabo , monba ngombe nadbweza pansi bobadwamo. 14 Kwanja kwanga kwatenga, muchisa, chuma cha maziko, ndipo ngatiumozi wasonkaniza ma eyesi yosiyiwa. Ninaunjika ka doti, kulibe anatambulula mapapiko, kapena kusegula pakamwa, kapena kujumpilami." 15 Kodi katemo kangazimvele kususana nabo kapanga? Chojubila chingazimvses kupambana uja wamene ajubilako? chili ngati ndodo inyemula baja bamene bainyemula. Monga ngati ndodo iyemula mutnu, wamene ayinyamula. 16 Kwaicho Ambuye Yehova wamakamu azatuma matenda pakati pabo patulidwa ankondo ake ndipo pansi paulemelelo wake ku zankala kuyasha kupya ngati mulilo. 17 Ku unika kwa Isilayelu kuzankala mulilo, ndipo oyela bake chimbili, chizapya ndipo nakuononga minga yake navochingiliza musiku limozi. 18 Yehova azashoka ulemelelo wa sanga yake nazabyala muntaka pamozi pamuzimu napatupi; azankala monga mwamene umoyo wamuntu wodwala umaila. 19 Mitengo yosala musanga zankala yochepa na mwana mungono, aza belenga. 20 Pasiku lija, osala a Isilayli banja la Yakobo yamwazikana, ibaza dalila amene azabagonjesa, kooma azadalila kwa Yehova, woyela wa Isilayeli. 21 Osala a Yakobo azabwelella kuli Mulungu wampamvu. 22 Ngankale bantu bako, Isilayeli, bali monga muchanga wakunyanja, bosala benve bazabwelela. Chiwonongeka chakambiwa monga chilungamo chotayikila ailamula. 23 Ambuye Yehova waakamu, azaltea chiwonogekeko chamene alingilila mumalo yonse. 24 Kwaicho Ambuye Yehova wa makumu akamba kuti, bantu banga bankala mu Zayoni, osayopa Asilia. Azakumenyani naimwe, monga anachita ba Igiputo. 25 Musamuyope enve, Mwakantawi kangono ukali eanga kususana naimwe kuzasila ukali wanga uzabasogolela kuchiwonongeko." 26 Ndipo Yehova wamakamu azasebenzesa mukwapu kususana nawo benve. Monga anagonjesa Midani pamwala wa Orebu. Azanyamula ndodo pa nyanja pa mwamba monga anachita ku Igipito. 27 Pasiku ija, cholema chizachosedwa papewa yako ndipo goli yake za chosewapo pamikosi yanu, ndipo goli izawonongeka kamba koina. ***kusilisa kwa malemba kwa ndime nik vuta chifukwa chilingana zolembedwa. kumusulila kwa sopano kusiyako chifukwa chaina, zimasulidwe zina zasopano zimen kuti goli lizawonongewa kuchosewa pamikosi yanu. Ayenda pa mwamba kuchokela kwa Rimoni. Apa atanatuza mfumu ya Asiliya na aakondo bake.*** 28 Ba dani babwela kwa Aiati anapita nakupyola ku Migironi, ku Mikimasi anasungila makatundu yake. 29 Anawoloka nakupita kugona ku Geba, Rama anatutuma na Gibiya wa sauli anataba. 30 31 32 Lilami mopunda, mwana mukazi wa Gelimu! Mvesesani, Laisha! naimwe bo sauka baku Anatoti! Siku yamene ija azaimisa pa nobu nakunyanganisa kwanja yake papili yabana ba kazi ba Zayoni lupili ya Yelusalemu. 33 Onani, Ambuye Yehova wamakamu azachosa musambo naku pwanya koyofya; mitengo zitali zizaduliwa pansi, ozikuza azabwezewa pansi Lebanoni mukuzimvela azagwa. 34 Azajuba visakasak vamusanga nakatemo, na Lebanoni ulemelelo wake uzagwa.