1 ndipo iwe, obadwa na munthu zitengele lupanga yakuthwa weka, naku pitisa kaleza mumutu naku devu zako, ndipo tenga sikeli ku apima naku siyanisa sisi yako. 2 Soka gawo imozi mogaba patatu mumulilo pakati pa muzinda pamene masiku yozugulukiwa yaka sila, naku tenga gawo imozi mwa magawo yatatu ya stsi yake naku kumenya na lupanga mozungulila mzinda. + Ndipo mwazya mo gaba patatu mu mphepo, + ndipo ine niza chosa lupanga kupilikisha banthu. 3 Koma tengako tsitsi in’ono pali izo, naku kumangilila mubali mwa chovala chako. 4 Ndipo tengani sisi yabili ndi kliponya pakati pa mulilo; naku kutaila pamulito; kuchokera kuja mulil uzayabukila mu nyumba yonse ya Isiraeli. 5 Ambuye Yehova akamba kuti, iyi ni Yerusalemu pakati pa amitundu, kwamene namuika, ndipo kumene munamuzuluka na maiko yena. 6 Koma eve wakana mau yanga moipa kupitilila mitundu yalinazo, na malemba anga kopitilila maiko yomuzunguluka.banthu bakana chiweruzo changa ndipo sanayende mumau yanga. 7 Cifukwa cace Ambuye Yehova akamba kuti chifukwa ndiwei obvuta kopitilila mitundu yokuzunguluka iwe siunayende mumalamulo yanga, kapena kucita monga mwamene mau yanga, kapena kucita monga mwamene mau ya mitundu bokuzugulukani; 8 cifukwa cace, Yehova, Ambuye akamba izi kuti, onani! Ine idzachita mosushana nawe. Niza weruzo pakati panu kuti mitundu ione. 9 Nizakuchitira zamene siinachitepo ndipo zimene sinidzachitafuti, chifukwa cha zonyansa zako zonse. 10 Cifukwa cace atate azadya bana pakati panu, na banab azadya batate bao; chifukwa nizakulanga naku mwazyani ku mbali zonse imwe nonse bosalako. 11 Cifukwa cace, malinga nili moyo akamba Ambuye Yehova popeza nichosimikiza kuti mwa ononga nyumba yanga yopatulika na zokalipisa zanu na zonyasisa zanu , kwakuti ine niza ku chepesani; menso yanga siyaza michitilani chifundo imwe, ndipo siniza kusiyani. 12 Umozii wa imwe azafa namatenda, ndipo baza sila najala pakati kanu. Umozi pakati kanu aza paiwa nalupanga mozugulukiwa. ndipo niza kumwazani ba tatu bali yosiyasiyana, naku chosa lupanga ku ba pilikisha na beve. 13 Pameneapo mkwiyo wanga uzasila, ndipo nizasiliza ukali wanga pali beve. nizakahala okutila, ndipo baziba kuti ine, Yehova, nakamba mokalipa nika siliza ukali wanga kuli beve. 14 Nizakuonogani nakuku chitisani soni ku maiko yokuzungulukani pameso pa aliyense bopita najila. 15 Ndipo Yerusalemu izakhala chinthu choweluziwa na banthu bena , nakuku sekani, chenjezondipo choyofya kuma maiko yokuzunguluka imwe. Nizaku weluzani imwe mumukwiyo na ukali, i na ukali okalipila-i Yehova achikamba ichi! 16 Nizatumiza mivi yoofiya za njala yamene ishushani na imwe. Pakuti nizakhala jila yoku ku onogelanikoni imwe. pakuti niza pakisa njala pali imwenaku chosapo buledi. 17 Nizakutumizirani njala na soka kuti mukhale opanda bana. matenda na magazi zidzadutsa pakati panu, ndipo nizakubwertserani lupanga imw-i, Yehova nazikamba izi.