Mutu 1 2

1 Ndipo tinabwelela na kutenga ulendo wathu mu chipululu mu njila yaku nyanja ya Reedis, monga Yehova anakambila kuli ine; tinayenda mozungulila pili ya Seir mu masiku yambili. 2 Yehova anakamba kuli ine, nakuti, 3 'mwayenda muzunguluka ili pili mwantawi itali; pindamukilani ku mumwela. =======