1
Ndipo tinabwelela na kutenga ulendo wathu mu chipululu mu njila yaku nyanja ya Reedis, monga Yehova anakambila kuli ine; tinayenda mozungulila pili ya Seir mu masiku yambili.
2
Yehova anakamba kuli ine, nakuti,
3
'mwayenda muzunguluka ili pili mwantawi itali; pindamukilani ku mumwela.
=======