Mutu 1

1 Aya ndiye mau yamene Mose anakamba kuli Israeli yonse kupitilila Yodano muchipululu, mu malo yalibe chilichonse ya mumana wa Yodano mu chikwa ca safu, pakati pa Parani, Toperi, Labani, Hezeroti, na Dizahabu. 2 Ni masiku ileveni ulendo kuchokela ku Horebu mu njila yaku pili ya Seira kufika ku Kadeshi Maniya. 3 Chinachitika mu chaka cha namba Fote, mu mwezi wa namba leveni, pasiku loyamba ya mwezi, kuti Mose anakamba ku banthu ba Isareli, kubauza vonse vamene Yehova anamulamulila iye pa zabeve. 4 Ichi chinali pambuyo Yehova anaononga Sihoni mfumu ya ma Amori, wamene anankhala mu Heshboni, na Og mfumu ya Bashan, wamene anankhala mu Ashtaroth ku Edrei. 5 Kupitilila mu Yodani, mu malo ya Moabu, Mose anayamba ku vumbulusa izi zofunikila, nakuti, 6 ''Yahova Mulungu wathu anakamba kuli ife pa Horebu, nakuti, 'Mwankala maningi muli iyi pili muziko. 7 Pindamukani nakuyabako ulendo wanu, nakuyenda ku ziko yapa pili ya baku Amori naku malo yonse yapa fupi nakuja mu malo yalibe chilichonse mu chikwa cha mumana wa Yodano, mu ziko yakumapili, mu malo yamunyansi, mu Negevi, nakumbali kwa mumana-malo yaba ku kenani, na ku Lebanoni mpaka kufika kumumana ukulu wa Efuletis. 8 Ona, naika malo pasogolo panu; yendani mukati naku tenga malo yamene Yehova analumbila kuli batate banu-kuli Abulahamu, kuli Isaki, na Yakobo-kupasa kuli beve na kuli mubadwe wao uzakonka beve. 9 Ninakamba na imwe pali ija ntawi, nakuti, 'Sinili okonzeka ku kutengani imwe mwaine neka. 10 Yehovah Mulungu wanu akupakisani imwe, onani, muli lelo monga zambili ntandala za kumwamba. 11 Lekani Yehova, Mulungu wa batate banu, akupangeni imwe ma sausandi monga mwamene mulili, na kukudalisani, monga mwamene anakulonjezani imwe! 12 Nanga ninga nyamule bwanji mitolo yanu ine neka, makatundu yanu, na mukangano wanu? 13 Tengani bamuna ba nzelu, bamuna bachinveseso, na bamuna ba mbili yabwino kuchoka ku mutundu uli onse, nizabapanga bosogolela pali imwe. 14 ' munaniyanka ine nakukamba, ' vintu vamene wakamba vili bwino kuli ife kuvichita.' 15 Mwaicho ninatenga basogoleli ba mitundu yanu, bamuna banzelu, na bamuna ba mbili yabwino, nakubapanga basogoleli pali imwe, boyanganila masausande, boyanganila ma handeledi, boyanganila ma fifite, boyanganila ma kumi, na bama udindo, mutundu pa mutundu. 16 Ninalamulila boweluza banu pa ntau ija, kukamba, ' Nvelani mikangano pali ba bale banu, nakuweluza molungama pakati muntu na mubalae wake, na mulendo wamene ali naye. 17 Imwe simufunika kulangiza kusanka ku aliyense ali mu kususana; imwe muzanvela mung'ono na wonveka molingana. Imwe simuzayopa maonekedwe ya mwamuna, chifukwa chiweluzo nicha Mulungu. Kususana kwamene kuli kovuta kuli imwe, muzambwelesa kwaine, ndipo ine nizanvela.' 18 Nikulamulilani pali ija ntawi vinthu vonse vamene mufunika kuchita. 19 Tinayenda kuchoka ku Horeb na kuyenda mukati monse mwa monveka na moyofya muchipululu chamene munaona, munjila yathu ku ziko yapapili ya Amori, monga Yehova Mulungu wathu anakambila; ndipo tinabwela ku Kadeshi Barbea. 20 Ine ninakamba naimwe, 'Mufunika kubwela ku lupili ya ziko ya Amori, yamene Yehova Mulungu wathu atipasa. 21 Onani, Yehova Mulungu wanu aika malo pasogogolo panu; yendani pamwamba, tengani malo, monga Yehova, Mulungu wa batate banu, akambila kwa imwe; simufunika kuyopa, kapena kunkala wokumudwa. ' 22 Aliyense pali imwe anabwela kuli ine nakukamba, 'tiyeni titume bamuna pasogolo patu, kuti banga tioneleko malo, nakutiletela mau mwamene tikamenyele nkondo, na mizinda yamene tizangenamo.' 23 Nkani iyi inanikondwelesa maningi; ninatenga bamuna tweovu pali imwe, mwamuna umozi kuchoka kumutundu uli onse. 24 Banabwela naku yenda kuziko yaku mapili, banabwela ku chikwa cha Eshikoli, naku ona ona. 25 Banatenga vina vipaso vamu ntaka mu manja mwawo nakuleta kuli ife. Banabwelensanso kwa ife mau na kuti, 'Ni malo yabwino yamene Yehova wathu Mulungu atipasa.' 26 Koma munakana kuukila, koma muna pandukila mosusana na malamulo ya Yehoha Mulungu wanu. 27 Munadandaula mu misasa yanu na kuti, ''Ni chifukwa kuti Yehova anatizonda ife kuti Iye abwelesa kwife kuchoka mu malo ya Igupto, kutipasa mukati mumanja ya Amori kutiononga ife. 28 Nikuti kwamene tinga yende manje? Bathu babale bapanga yathu mitima kusungunika, kuti, 'Awo bathu ni bakulu na batali kuchila mwamene tilili; Minzi yawo ni ikulu ndipo niyolimba kufika kumwamba; koma, tababona bana bamuna ba Anakimu kuja.'' 29 Ndipo ninakamba kuli imwe, 'Musankale na manta, kapena musayope beve. 30 Yehova Mulungu wanu, wamene ayenda pasogolo panu, azakumenyelani, monga vilivonse vamene anachita kuli imwe mu Igupto pamenso panu, 31 na futi muchipululu, kwamene munaona mwamene Yehova Mulungu wanu anakutengelani, monga mwamuna atengela mwana wake mwamuna, kulikonse kwamene munayenda kufikila munabwela kuli yano malo.' 32 Koma ngankale aya mau simunakulupilile Yehova mulungu wanu, 33 analikuyenda pasogolo panu kukupezelani malo imwe yapangilapo musonkano, mumulilo usiku na mukumbi muzuba. 34 Yehova ananvela chongo cha mau yanu na kukalipa; analapa na kuti, 35 'Zoona kulibe umozi wa aba bamuna bauyu mubadwe wochimwa uzaona yabwino malo yamene ninalumbila kupasa makolo yanu, 36 kuchosako Kalebu mwana mwamuna wa Jephunneh. Azaiona ndipo nizamupasa iye na wobadwa mumalo yamene anadyakamo, chifukwa anamukonka Yehova.' 37 Komanso Yehova anali wokalipa naine chifukwa cha imwe, nakuti, 'Naiwe siuzayenda kuja; 38 Yoswa mwana mwamuna wa Nuni, wamene aimilila pasogolo panu, azayenda kuja; mulimbikiseni, chifukwa azasogolela Israeli kuti batenge malo. 39 Komanso, bana banu bang'ono, bamene munakamba kuti bazankala wozunzika, bamene lelo balibe nzelu za bwino kapena zoipa - bazayenda kuja. Kuli beve nizabapasa, ndipo bazatenga kunkala yawo. 40 Koma imwe, pindamukani na kutenga ulendo wanu mu chipululu kupitila mu njila yaku nyanja ya Reedis.' ======= 39 Elo, bana banu ban'gono, bamene munakamba kuti baza vutikilamo, bamene lelo balibe nzelu zoziba chabwino na choipa-bayenda kungeni muja. Kuli beve nizaba pasa, ndipo yazankala yao. 40 Koma kwaimwe, pindamukani nakuyambako ulendo wanu muchipululu mubali mwanjila yaku mumana wa Reedi.' >>>>>>> 31f2266056f1a583193e6f4b2d0ffec4c1748c84 41 Ndipo munaniyanka na kuti, 'Tachimwa mosusana na Yehova; tizayenda na kumenyana, ndipo tizakonka vonse vamene Yehova Mulungu wathu atilamulila ife kuti tichite.' Aliyense mwamuna muli imwe avale zida zake zankondo, ndipo munali okonzeka ku gonjesa ziko yapapili. 42 Yehova anakamba kuli ine, 'Kamba kuli beve, ''musaukile na osamenya, chifukwa sinizankala na imwe, ndipo muzagonjesedwa kuli badani banu.' ======= 41 Mwaicho muna yanka nakukamba kuli ine, ' Tachimwila Yehova; tizayenda nakumenya bantu bamumalo yaja, ndipo tizakonka vonse vamene Yehova mulungu watu alamulila ife kuchita.' Mwamuna aliyense pali imwe avale chida chake cha nkondo, mwaicho munali bkonzeka kumenya ziko yaku mapili. 42 Yehova anakamba kuli ine, ' kamba kuli beve, '' Musachite ndeo kuli aba bantu nakubamenya, chifukwa sinizankala na imwe, mwaicho muzamenyewa naba dani banu.' >>>>>>> 31f2266056f1a583193e6f4b2d0ffec4c1748c84 43 Ninakamba kuli imwe muli iyi njila, koma simunanvele. Munapanduka mosusana na malamulo ya Jehova; Munali ozikuza na kuukila ziko yapapili. 44 Koma ma Amori, bamene banankala pa ziko yapapili, banabwela mosusana naimwe na kukupilikishani monga nzimu, na kumenya imwe pansi mu Seir, kutali monga ku Hormah. 45 Munabwela na kulilila pamenso pa Yehova; Koma Yehova sananvele ku mau yanu, kapena kuponyako nzelu kuli imwe. 46 Ndipo munankala mu Kadeshi masiku yambili, yonse masiku yamene munankala kuja. ======= 45 Munabwelela naku lila pamenso pa Yehova; koma Yehova sananvele mau yanu, olo kuikilako nzelu kuli imwe. 46 Mwaicho munankala ku Kadeshi masiku yambili, yonse masiku yamene munankala kuja. >>>>>>> 31f2266056f1a583193e6f4b2d0ffec4c1748c84