1 Vinachitika mu mwaka wa naini olamulila wa Zedekaya, mu mwezi wa nambala teni, pa siki ya nambala teni ya mwezi, Nebuchadneza mfumu wa Babiloni anabwela gulu ya bankondo ku Jersaluma. Anamanga misasa pandunji pake, banamanga koma lozungulila. 2 Chakuti muzinda bana wungulaka kufikila mu mwaka wa nabmbala ileveni wo lamulila kwa mfumu Zedekaya. 3 Pa siku la nambala nani mu mwezi wa nambala fo wa mumwaka uja, njala inali ikulu mumuzinda chakuti banalibe chokudya mumalo. 4 Pamene muzinda banaungenela, bamuna bankondo bonse banataba usiku yabili, ku munda wa mfumu, kale bakalonga banali kuzinguluka muzinda. mfumu anapita ku mbali yama Araba. 5 Koma gulu a nkondo yaba kalongo anapilikisha mfumu Zedekaya nakumupeza mumalo yalibe Jericho. Gulu yankondo yake yonse masalangana kuchoka kuli enve. 6 Bana gwila mfumu na kumuleta mu Babiloni lu Riblah, kwamene bana peleka weluzzo pali enve. Ku bana ba Zedekaya, bana ba paya pamenso apke. 7 Ndipo anamuchosa menso, nakumanga na unyolo ya bronzi, nakumuleta ku Babiloni. 8 Mu mwezi wa nambala faivi, pa siku ya nambala seveni ya mwezi, unali mu mwaka wa nayintini wa lamulila wa Nebukadineza mfumu ya Babiloni, Nebukadineza, kapolo wa mfumu ya Babiloni na musogoleli wa oteteza, bana bwela ku Jerusalema. 9 Anashoka nyumba ya Yehova, nyumba yachifumu, na manyumba yonse yamu Jerusalema; nanyumba zonse zofunisaka maningi mu muzinda anashoka. 10 Makoma onse ozingulukila Jerusalema, yonse gulu ya nkondo ya bamu Babiloni banali pansi pamu sogoleli wabo teteza anaba wononga. 11 Bantu benangu bonse banasala mumuzinda baja banasiya mfumu ya Babiloni, nabe banasala-Nebuzaradan, musogoleli wabo teteza, anabapeleka mukubanga. 12 Koma musogoleli wabo tetezea anasiya bosauka muminda. 13 Kuzi pilala za bronzi zinali munyumba ya Yehova, na maimidwe, na nyanja ya bronzi inali munyumba ya Yehova, ba kalongo banaz pwanya muzi dunswa dunswa na nyumba bronzi kuibweze ku Babiloni. 14 Ma poto, ma fosholo, wokonza nyali, suouni, nazonse ziwiya za bronzu zamene wansembe anali kwebezensa mu tempele-ba kalonga bana vichosa. 15 Ma poto yochosela miloto namabale yanali yopangiwa na golide, nayo pangiwa na siliva-ba kapitawo babo teteza mfumu banavi tenge navenve. 16 Ma pilala yabili, nyanja, namaimidwe yamene Solomoni enze anapanga mu nyumba ya Yehova ina na bronzi yambili kuchila inapimiwa. 17 Utali bwa pilala yoyambila inali eyitini mikono, ndipo mutu wa bronzi unali pamwamba. Mutu unali mikono itatu mubutali, na latticework na makangaza kuzunguluka mutu onse, zonse zenze zo pangiwa na bronzi. Ma pilala yenangu nama latticework yawo yanali monga yo yambila. 18 Musogoleli wabo teteza atenga Seraia mukulu wansembe, pamozi na Zefaniya, nsembe wachibili, ba malonda ba pachipata batatu. 19 Kuchokela mumuzinda anamangisa mukulu analikuna asilikali, bamuna bali faivi banali kulangiza mfumu, banali mumuzinda. Anamangisa mukulu wa gulu yankondo ya mfumu anali wodalilika kulemba bamuna bamu gulu yankondo , pambali nabamuna bofunika maningi bali sikisite bamu malo banali mumuzinda 20 Pamene Nebuzaradan, musogoleli wabo teteza, anabatenga nakubaleta kuli mfumu wa Babiloni ku Riblah. 21 Mfumu wa Babiloni anabapaya ku Riblah mumalo ya Hamath. Munjila iyi, Yuda anachoka mumalo yake mukumangisidwa. 22 Kubantu bamene banasala mumalo ya Yuda, bamene Nebukadineza mfumu wa babiloni anasiya, anafaka Gedaliya mwana wa Ahikam, mwana wa Shafan, kubayangana. 23 Manje pamene bonse b asogoleli ba asilikali, benve naba muna bawo, bananvela kuti mfumu wa Babiloni anafaka Gedalia kazembe, banayenda kuli Gedalia mumuzipa. Bamuna aba banali Ishmael mwana wa nethaniah, Johanani mwana wa Kareah, Seraiah mwana mwamuna wa Tanhumeth netofatite, na Joazaniah mwana wa Makkatite- benve nabantu babo. 24 Gedaliah anapanga lamulo kuti benve na bantu babo, anakamba kuti kuli benvd, "musayope akulukulu alalonga. Nkani mumalo na kutumikila ya Babiloni, ndipo vizankanla mushe naimwe." 25 Koma vinachitika kuti mumwezi wa namabala seveni Ishmael mwana wa Nethaniah mwana wa Elishana kuchokela ku banja lachifumu, anabwela nabamuna teni naku kukira Gedaliah. Gedaliah anafa, kumozi na bantu ba Yuda naba mu Babiloni banali nainve ku Mizpa. 26 Pamene bantu bonse, kuchokela kufika kubakulu, na baogoleli ba asilikali, ba nanyamuka nakuyenda ku Iguputo, chifukwa banali kuyopa bamu Babiloni. 27 Zinachitika kusogolo mu mwaka wa sate-seveni waku mangiwa kwa Jehowatini mfumu ya Yuda, mu mwezi wa nambala twelufu, pa siku la twenti seveni la mwezi, pamene Awel-Maduku mfumu wa Babiloni anachosa Yehowatini mfumu wa Yuda wa Babiloni anachosa Yehowatini mfumu wa Yuda mu ndende. Ivi vinachitika mumwaka wamene Awel-Maduku anayamba ku lamulila. 28 Anakamba mushe kuli enve nakumupasa mupado olemekezeka kuchila ya mfumu zinangu zinali na enve mu Babiloni. 29 Awel-Maduku anachosa vovala va Yehowatini zanu ndende,ndipo Yehowakin anadya ntawi zonse pa tebulo mfumu kwa moyo wake wonse. 30 Anali ku pasiwa malipilo ya vokudya masiku onse kwa moyo ake onse.