Mutu 6

1 Bana bamuna ba Levi banali Geshoni, Kohati, na Merari. 2 Bana bamuna ba Kohati benzeli Amramu. Iza, Heberoni, na Uzziel. 3 Bana ba Amramu benzeli Aroni, Mose, na Miriamu. Bana bamuna ba Aroni benzeli Nadabu, Abihu, Eleaza, na Itama. 4 Eleaza anankala tate wa Finyasi, na Finyasi anankala tate wa Abishua. 5 Abishua anankla tate wa Buki, na Buki anankala tate wa Uzzi. 6 Uzzi anankala tate wa Zeraya, na Zeraya anankala tate wa Merioti. 7 Merioti anankala tate wa Amaria, na Amaria anankala tate wa Ahitubu. 8 Ahitubu anankala tate wa Zadoku, na Zadoku anankala tate wa Ahimazi. 9 Ahimazi anankala tate wa Azarria, na Azaria anankala tate wa Yohanani. 10 Yohanani anankala tate wa Azaria, wamene anali opelekela mu chalich yamene Solomoni anapanga mu Jerusalema. 11 Azariya anankala tate wa Amariyah ndipo Amariyah anankala tate wa Ahitubi. 12 Ahitubi anankala tate wa Zadoki, na Zadoki anankala tate wa Shalumu. 13 Shalumu anankala tate wa Hilikiya, ndipo Hilikiya anankala tate wa Azariya. 14 Azariya anankala tate wa Seraya, na Seraya anankala tate wa Jozidaki. 15 Jozidaki anangena mundende pamene Yehova anafaka mu undende Yuda na Jerusalema na kwanja ya Nebuchadineza. 16 Bana bamuna ba Levi benzeli Geshoni, Kohati, na Merari. 17 Bana bamuna ba Gershoni banali Libni na Shemayi. 18 Bana bamuna ba Kohati banali Amuramu, Izam=, Heberoni, na Uzziel. 19 Bana bamuna Merari banali Mahli na Mushi. Aya ndiye ma banja ya ba Levi molingana na batate babo. 20 Ba mubadwe wa Geshoni: Libini mwana wake mwamuna , Yahati mwana wake mwamuna, zina mwana wake mwamuna, 21 Yowa mwana wake mwamuna, Iddo mwana wake mwamuna na Yeteraiyi mwana wake mwamuna. 22 Ba mubadwe wa Kohati: Aminadabi mwana wake mwamuna, Kora mwana wake mwamuna, Asiri mwana wake mwamuna, 23 Elikana mwana wake mwamuna, Asiri mwana wake mwamuna, 24 Tahati mwana wake mwamuna, Uriyele mwana wake mwamuna, Uzzia mwana wake mwamuna, na Shaul mwana wake mwamuna. 25 Ba mubadwe wa Elikana banali Amasai, Ahimoti, 26 Elkana mwana wake mwamuna, Zofayi mwana wake mwamuna, Nahati mwana wake mwamuna, 27 Eliabu mwana wake mwamuna, Jerohamu mwana wake mwamuna, na Elkana mwana wake mwamuna. ***kumasula kwakudala kuma kwachi Geriki kuma pamudadada Samueli mwana wake.*** 28 Bana bamuna ba Samueli banali oymaba kubadw Yoweli, na Abiya,Wachibili kubadwa. 29 Ba mubadwe wa Merari banali Mali, Libni mwana wake mwamuna, SHimeyi mwana wake mwamuna, Uza mwana wake mwamuna. 30 Shimya mwana mwamuna, Haggai mwana wake mwamuna, na Asaya mwana wake mwamuna. 31 Aya ndiye mazina ya bantu bamene Davide ana ika muku yanganila pali nyimbo mu nyumba ya Yehova, pamene bokosi ya chipangano inbwela mwamene mufa. 32 Banali kupeleka mo yimba pasogolo ya chalichi, mu hema ya musonkano kufikila pamene Solomoni anapangila nyumba ya Yehova mu Jerusalema. Bana fikiliza nchito zabo monga kuli malamulo bana pasiwa. 33 Aba banali baja botumikila pamozi na bana babo bamuna. Hemeni oymiba anacokela ku ma banja yaba kohati. Aba banali makokolo yake, kubwelela mu ntawi ya kumbuyo: Hemani anali mwana mwamuna wa Yowele. Yowele anali mwana mwamuna wa Samueli. 34 Samueli anali mwana mwamuna wa Elikana. Elikana anali mwana mwamuna wa Eliyele. Eliyele anali mwana mwamuna wa towa. 35 Towa anali mwana mwamuna wa Zufu. Zufu anali mwana mwamuna wa Elikana. Elikana anali mwamuna wa Mahati. Mahati anali mwana wa Amasayi. Amasayi anali mwana mwamuna wa Elikana 36 Amasayi anali mwana mwamuna wa Elikana. Elikana anali mwana mwamuna wa Yowele. Elikana mwanna mwamuna wa Azariya. Azariya anali mwana mwamuna wa Zefaniya. 37 Zefaniya anali mwana mwamuna wa Tahati. Tahati anal mwana mwamuna wa Asiri. Asiri anali mwana mwamuna wa Ebiyasafu. Ebiyasafu anali mwana mwamuna wa Kora. 38 Kora anali mwana mwamuna wa Iza. Iza anali mwana mwamuna wa Kohati. Kohati anali mwana mwamuna wa Levi. Levi anali mwana mwamuna Isilayeli. 39 Hemani muzake anali Asafu, wamene anali kuimiulila ku kwanja ya kumanja yake. Asafu anali mwana mwamuna wa Brekiya. Berekiya anali mwana mwamuna wa Simiya. 40 Simiya anali mwana mwamuna wa Mikaele. 41 Mikaele anali mwana mwamuna wa Baaseiya. Baaseiya anali mwana mwamua wa Milikiya. Milikiya anali mwana mwamuna wa Etini. Etini anali mwana mwamuna wa wa Zera. Zera anali mwana mwamuna wa Adaya. 42 Adaya mwana mwamuna wa Etani. Etani anali mwana mwamuna wa Zima, Zima anali mwana mwamuna wa Simiya. 43 Simeyi anali mwana mwamuna wa Yahati. Yahati anali mwana mwamuna wa Levi. 44 Ku kwanja ya manzere ya Hemani kunali ba nzake bana ba Merari. Bana patikizapo Etani mwana mwamuna wa Kisi. Kisi anali mwana mwamuna wa Abidi. Abidi anali mwana mwamuna wa Maluki. 45 Maluki anali mwana mwamuna wa Hasabiya. Hasabiya anali mwana mwamuna wa Amaziya. Amaziya anali mwana mwamuna wa Hililkiya. 46 Hilikiya anali mwana mwamuna wa Amuzi. Amuzi anali mwana mwamuna wa Bani. Bani nali mwana mwamuna wa Sema. 47 Sema anali mwana mwamuna wa Mahili. Mahili anali mwana mwamuna wa Musi. MUsi anali mwana mwamuna wa Merari. Merari anali mwana mwamuna wa Levi. 48 Ba bweniz babo, ba Leviti, bana tumimikiziwa kuchita nchito zonse zamu kachisi., nyumba ya Mulungu. 49 Koma Aroni na bamu badwe wake bana pelkea vopeleka pa guwa ya nsembe zofunkiza pa nchito zonse pa malo chitetzero cha Isilayele, monga kuli vonse vamene Mose mutumiki wa Mulungu ana lamulila. 50 Bamubadwe wa Aroni nibo pendeka monga vonkampo: mwana mwamuna wa Aroni anali Eleyazari. Mwana mwamuna wa Eleyazari a ali Finehasi. Finehasi anali mwana mwamuna wa Abishuwa. 51 Mwana mwamuna wa Abishuwa anali Buki mwana mwamuna wa Buki anali. Uzi mwana wake mwamuna anali Zerahiya. 52 Zerahiya mwana wake mwamuna anali Merayoti. Merayoti mwana wake mwamuna anali Amaraya. Amaraya mwana wake mwamuna anali Ahitubi. 53 Ahitubi mwana wake mwamuna anali Zadoku. Zadoku mwana wake mwamuna anali Ahimazi. 54 Aya ni malo yamene ba mubadwe wa Aroni bana pasiwa ku kunkalamo kukamba kuti. bamubadwe wa Aroni bamene banali kuchokela ku ma banja yama Kohati ( malo yo yamba yanali yabo). 55 Kuli benve bana pasiwa Heberoni mu ziko ya Yuda na malo yake yodyeselako vibeto, 56 koma minda za mu muzid na minzi zake banapasa Kalebu mwana mwamuna wa Yefune. 57 Kuli bamubadwe wa Aroni banapasa Heberoni (muzinda yopulumikilamo, na LIbina pamozi na malo yake yodyeselako. Bibeto, Yatili, Estitemowa na malo yake yodyeselako vibeto, 58 Hileni na malo yake yodyeseleko vibeto, na Debriri pamozi na mali yake yodyeselako vibeto. 59 Bana pasako na kuli ba munadwe ba Aroni: Ashani na malo yake yodyeselako vibeto, Yuta, ***zina ya malo Yuta mulibe mu mabaibulo yachi koma ipezeka m kumasulila kwa siriyaki kwama kope yama Heber: onanikoni na Yoswa 21:16*** na Beth Shemesi na malo yake yodyeselako vibeto; 60 na kuchokela ku mutundu wa Benjamini, Geba na modyeselako vibeto mwake. Alemeti pamozi modyeselako vibeto, Anatoti pamozi na modyeselako mitundu zonse zinali mizinda 61 Kuli bonse bamubadwe ba Kohati, bana pasiwa mizinda kumi kuchokela ku mutundu ogabika pakati wa Manase. 62 Kuli bamubadwe ba Geshoni muma banja yabo yosiyana siyana bana pasiwa mizinda fetini kuchokela ku mitundu zaku Isaka, Asere. Nafutali naba mutundu wo gabika wa Manase mu Basani. 63 Kuli ba mubadwe wa Merar bana pasa mizinda twelevu, banja, kuchokela kuli mitundu za Rubeni, Gadi, na Zebulani. 64 Mwaicho bantu baku Isilayele banapa izi mizinda pamozi na modyesela vobeta mwao kuli ba Levi. 65 Bana pasiwa mwa maere ma tawani ya kambiwa poyamba kuchokela ku mitundu zaba YUda, Simiyoni, na Benjamini. 66 Ma banja yena yaba Kohati yana pasiwa mizinda kuchokela ku malo ya mutundu wa Efuremu. 67 Bana bapasa: Shekemu (muzinda wopelumukilamo) pamozi na modyesela vibeto mwake muzio yama pili ya Efaremu, Gezere pamozi na modyesela vibeto mwake, 68 Yokomeamu na modyesela vibeto mwake Beti Horani na modyesela vibeto mwake, 69 Ajaroni na modyesela vibeto mwake, na Gati Rimoni na modyesela vibeto mwake. 70 Mutundu wogabikika pakati wa Manase una pasa ba Hohati Aneri na modyesela vobeta mwake na Birleamu na modyesela vobeta mwake. Ivi vinankala vintu va mabanja yene yonse yaba Kohati. 71 Kuli bamubadwe ba Geshoni bochokela muma banja yo gabika pakati ya Manase, bana ba pasa Golani mu Bashani na modyesela vibeto mwake na Ashtaroti na modyesela vibeto mwake. 72 Mutundu wa Isaka unapasa kuli bamubadwe ba Geshoni Kedeshi na modyesela vibeto mwake, Daberati na modyesela vibeto mwake. 73 Ramoti na modyesela vibeto mwake, na Anemu na modyesela vibeto mwake. 74 Isaka analandila kuchokela ku mutundu wa Asheri: Mashali na modyesela vibeto mwake, Abudoni na modyesela vibeto mwake. 75 Hukoki na modyesela vibeto mwake, na Rehobi na modyesela vibeto. 76 Bana landila kuchokela ku mutundu wa Nafutali: Kedeshi mu Galileya na modyesela vibeto mwake, na Hamoni na modyesela vibeto mwake, na Kiliyataimu na modyesela vibeto mwake. 77 Basala ba mubadwe wa Merari bana landila kuchokela ku mutundu wa Zebulani: Yokineamu, Kartahi, *** na Rimono na modyesela vibeto mwake; 78 ndipo kuchokela ku mutundu wa Rubeni, kuchuluka Yodani ku maba ya Yeriko, bana landila Bezeri mu zemba, Yahazi, 79 Kedemoti na modyesela vibeto mwake, na mafati na modyesela vibeto mwake. 80 Ba Levi bana landila kuchokela ku mutundu wa Gadi: Ramoti mu Geliyadi na modyesela vibeto mwake, Mahanaimu na vineto mwake, 81 Hesiboni na modyesela vibeto mwake, na Yazeri na modyesela vobeto mwake.