Mutu 5

1 Bana bamuna ba Rubeni mwana oymaba wa Isilayeli-manje Rubeni anali mwana oyamba wa Isilayeli, koma udindio waku badwa kwake unapasiwa kubana bamuna ba Yosefe mwana mwamuna wa Isilwayeli chifukwa Rubeni anachita choipa ku chivaka chaba tate bake ndipo sicholembewa ktui anali mwana mwamuna mukulu. 2 Yuda ndiye anali wampabuyo pa balongo bae bonse, ndipo anakala musogoleli. koma udindo wakubadwa wenze na Yosefe- 3 bana bamuna ba Rubeni, mwana oyamba wa Isilayeli beze Hanoki, Palu, Hezroni, na Karmi. 4 Bobadwa mumbuyo ba Yoweli benzeli: Yoweli mwana mwamuna wake enzeli Shemaya. 5 Shemaya mwana mwamuna wake enzeli Gogi. Gogi mwana mwamuna wake enzeli Reya. Reya mwana wake mwamuna enzeli Baal. 6 Baal mwana wake mwamuna enzeli Beera, wamene Tiglati-Pileser mfumu ya Assyria anatenga ku ukapolo, Beera anali musogoleli wa mutundu wa Rubeni. 7 Beera bachi bululu kulinga nama banja yabo, ba nalembewa mokonka ma banja: Jeieil musogoleli, Zekariya, na 8 Bela mwana mwamuna wa Azazi mwana mwamuna wa Shema mwana mwamuna wa Joel. Banakala mu Aroer, kufikila ku Nebo na Baal Meoni, 9 ndi kumawa kufika koyambila chipululu chofuka ku musinje wa Yufrate, chifukwa zibeto zabo zinali zapaka kwambili mumalo ya Geleadi. 10 Mu masiku ya Saulo, mutundu wa Rubeni wa unaukila ma hagriti nakuba gonjesa. Banakala mu malo yonkalamo ma yonse yakumwa kwa Gileadi. 11 Ma membala ba mutundu wa Gadi banankala pafupi na benve, mumalo ya Bashani kufikila ku Saleka. 12 Joel enzeli musogoleli; Shafamu anali wa namba tu; na Janai ndi Shafati mu Bashan. 13 Babululu babo, kama banja yaba tate babo, benzeli Michale, Meshullamu, Sheba, Jorai, Jakani, Zia, na Eba-bonse pamozi seveni. 14 Aba banut bakambiwa pamwamba benzeli bobadwa mumbuyo mwa Abihail, na Abihail anali mwana mwamuna wa Yuri. Yuri anali mwana mwamuna wa Jaroah. Jaroah anali mwana mwamuna wa Gileadi. Gileadi anali mwana mwamuna wa Michael. Michael anali mwana mwamuna wa Jeshishai. Jeshishai anali mwana mwamuna wa Jahdo. Jahdo anali mwana mwamuna wa Buzi. 15 Ahi mwana mwamuna wa Abdiel mwana mwamuna wa Guni, anali mukulu wama banja yaba tate babo. 16 Banankala mu Geleadi, mu bashani, mu muzinda yake ndi mumalo yonse yodyesela yaku Sharoni kufikila ku malile. 17 Vonse ivi vinzel volembewa mumitundu muma siku ya Jtamu mfummu ya Yuda na Jerobowamu mfumu ya Isilayeli. 18 Ma Rubeniti, ma Gadites, ndi pakati mutundu benzeli ya Manase 44,760 bopunzisiwa zankondo, banali kunyamula zishango na mikondo, na mibvii. 19 Bana ukila ma Hagritis, Jeta, Nafish, na Nodabu. 20 Bana landila tandizo yaumulungu kususana nabo. Mwa lehi, ma Hagriti na bonse bana gonjesewa chifukwa ba Isilayeli banalilila kuli Mulungu mu nkondo, ndipo anakulupilila chabo muli yenve. 21 Bana tenga nyama, kuikilapo fifite sauzande ngamela, 250,000 mbelele, tu sauzandi mabulu na 100, 000 bamuna. 22 Bambili banagwa cifukwa ndeo inali yachoka kuli Mulungu. Banankala mu malo mwao kufikila ukapolo. 23 Pakati mutundu wa Manasa banankala mu malo mwao kufikila ukapolo. Pakari mutundu wa Manase banankala mu malo ya Bashani Kufikila ku Ball Hermon na Seir (Iyo npili ya Hermoni). 24 Aba ndiye benzeli bakulu ba manyumba yaba tate bao; Efaa, Ishi, Eliel, Azreil, Yelemaya, Hodama, na Jadel. Bezenzeli bamuna bampavu, bamuna bazibika, bakulu bama nyumba ya baba tate babo. 25 Koma benxeli bosakulupilila kuli Mulungu wama kolo babo. Chifukwa benzeli kupempela tumilungu twabantu ba mumalo, bamene Mulungu anaononga kale. 26 Mulungu wa Isilayeli anaimisa Pul mfumu ya Assyria (ozibako futi Tiglati-Pileser, mfumu ya Assyria). Anatenga ukapolo ma Rubenites, Gadites, ndi pakakti pa mutundu wa Manase. Anabawelesa ku Halah, Habor, Hara, na kumusinje wa Gozani, kwamene bali kufikila siku yalelo.