Mutu 10

1 Manje ma Filistine bana menyana nama Isilayeli. Mwamuna aliyense waku Isilayele anataba kuchokela pali ma Filisti na kugwa pansi okufa pa lupili ya Gilibowa. 2 Ba Filisti bana pilikisha maningi Saulo na mwana mwamuna, Filisiti bana paya Yonatani, Abinadabu, na Maliki-Suwa, na bana bake bamuna. 3 Nkondo inamukulila Saulo, ndipo bopanga mivi banamu peza ndipo banamu panga vilonda. 4 Kuchokapo Saulo anakamaba kuli onyamula zida zake. "Chosa lupanga yako nakunilasa nayo. Ngati si ivo, aba bosa dulidwa baza bwela kuni vutisa." Koma onyamula zida zake sanacivhite, chifukwa anali na manta maningi. Mwaicho Saulo anatenga lupanga yake nake gwelapo. 5 Pamene onyamula zida zake anaona kuti Saulo anafa, anagwela pa lupanga yake nayenve na kufa. 6 Chakuti Saulo anafa, na bana bake bamuna batatu, chakuti na bonse bamunyumba mwake banafela pamozi. 7 Pamene bonse bamuna ba ku Isilayeli mu minda banaona kuti banataba na kuti Saulo na bana bake bamuna banafa bana siya mizinda zabo naku taba. kuchokela apo ba Filisti bana bwela natu nkalamo. 8 China bwela mozungulikila siku yokonkapo, pamene ma Filisti bana bweka kuvula bokufa, naku peza Saulo na bana bake bamuna banagwa pa lupili ya Gilibowa. 9 Bana muvula naku tenga mutu wake na zido zake. Bana tuma batumiki mu Filisiti yonse kupeleka nkani kuli tumilungu twao na kuli bantu. 10 Banaika zida zake mu chalichi ya milungu zabo, na kumangilila mutu wake kuli chalichi ya Diragoni. 11 Pamene ba Yabesi Gileyadi bonse bana nvela vonse vamene ma Filisti bana chit kuli Saulo. 12 Bonse bomenya nkondo bana yenda naku tenga tupi ya Saulo naya bana bake bamuna, naku yaleta kuli Yabesi. Bana shika ma bonzo yabo pansi pa mutengo mu Yabesi dipo sibanadye masiku seveni. 13 Chakuti Saulo anafa chifukwa enve anali osakululupilika kuli Yehova. Sanamvele malamulo ya Yehova, koma anafunsa malangizo kuchokela kuli muntu wamene anali kukamba na bokufa. 14 Sana pempe chisogozo kuchokela kuli Yehova, chakuti Yehova anamupaya naku pasa ufumu kuli Davide mwana ea Yesse.