1 Ndipo kumwamba na ziko yapasi zinalengedwa, na onse vintu vamoyo, vamene vinazulamo. 2 Pa siku ya seveni mulungu anasiliza nchito zamene enzeli kuchita, ndiponso ana pumula pa siku ya seveni ku nchito yake yonse. 3 Mulungu anandalisa siku ya seveni na kuyi patula chifukwa musiku yakaena anapumula kuchoka ku nchito zake zonse zamene anachita mukulenga kwake. 4 Ivi ndiye vinachitika pa zaka mwamba napa za ziko ya pansi, pamene vina lengewa, pa siku yamene Yehova Mulungu anapanga ziko yapansi na kumwamba. 5 Panalibe sanga paziko yampasi, ndipo panalibe vomela vamu sanga vamene vina choka, chifukwa Mulungu sana lengese mvula kuloka paziko yapasi ndipo kunalibe muntu olima pa ntaka. 6 Koma mame unaima kuchoka pa ziko ya pansi ndipo unatilila pamwamba pa ntaka. 7 Yehova Mulungu anapanga munthu kuchokela ku doti yapansi, ndipo anamupemela mumpuno mpepo ya umoyo ndiponso munthu anankala wamoyo. 8 Yehova Mulungu anashanga munda ku maba mu Eden ndipo mwamene muja anaikamo munthu wamene anapanga. 9 Kuchokela kudoti yapasi Yehova Mulungu analengesa mutengo ulionse ku kula zo oneka ku menso ndipo za bwino kudya. Kufakilako na mutengo wa moyo unali pakati pa munda, ndipo na mutengo wa kuziwa chabwino na choipa. 10 Mumana unachokela mu eden kutila munda. Kuchokela ado, unagabikana ndipo unankala mumana zili fo. 11 Zina ya mumana oyamba ni Pishon, ndiye yamene iyenda ku malo yonse ya Havilah kwamene kuli Golide. 12 Golide ya pa malo paja niya bwino. Pamalo paliko na Bdellium na mwala wa Onikisi. 13 Zina ya mumana wa chibili ni Gihoni. Weve uyenda mu malo yonse ya kushi. 14 Zina ya mumana wachitatu ni Tigirisi, ndipo uyenda ku maba kwa Ashuri mumana wa namba fo ni Euferetesi. 15 Yehovah Mulungu unatenga mwamuna naku muika mu munda wa Edeni kuti azisebenzamo naku sungamo. 16 Yehova Mu analamulila mwamuna, kuti, " Ndiwe omasuka kudya kuli mutengo uli onse wa m'munda. 17 Koma kuchokela mu mutengo oziba vabwino na voipa osadya, chifukwa siku yamene uzakadyako, zoona zoona uzaka mwalila." 18 Ndipo Yehovah Mulungu anakamba, " Sichabwino kuti mwamuna ankale Eka. Niza mupangila omutandiza omu wamila." 19 Kuchokela ku doti, Yehovah Mulungu anapanga nyama zonse zamuziko na nyoni zonse za mumwamba. Ndipo anavibwelesa kuli muntu kuona vamene azaviyitana chili chonse chamene muntu anaitana chilengedwe chaimoyo chili chonse, yamene iyo yenze zina. 20 Muntu anapasa mazina ku vobeta vonse, ku kuinyoni zonse za mumwamba, ndipo naku nyama zonse zammu zanga. Koma kuli mwamuna eve kunalibe anapezeka omutandiza omulinga. 21 Yehovah Mulungu analengesa muntu kuti angone tulo tukulu ndipo mwamuna anangona. Yehovah Mulungu anatenga mbambo imozi ya mwamuna naku valapo pa malo ya tupi pene anatenga Mbambo. 22 Na mbabo yamene Yehovah Mulungu anatenga kuli mwamuna anapanga mukazi na kumubwelesa kuli mwamuna. 23 Mwamuna akamba " Manje apa, iyi ni bonzo yama bonzo yanga, na tupi ya tupi yanga. Aza itaniwa mukazi chifukwa ana chokela kuli mwamuna." 24 Chifukwa cha icho mwamuna aza choka panyumba ya batate bake naba mai bake no kubwela pamozi na mukazi wake ndipo babili aba baza panga tupi imozi. 25 Bonse babili mwamuna na mukazi wake banali chitako koma sibenzeli kunvela nsoni.