1 Kale lidalipo mau ndi mau lidali pamoji nde Mulungu ndi mau wadali Mulungu. 2 Uyu mau kale wadali palimoji ndi Mulungu. 3 Vinthu vonchi vidachitika kupitila iye ndi palibe iye palibe hata chinthu chimoji ichochidali chachitika. 4 Mkati mwake mdali umoyo, ndi umene umoyo udali dangalila la wantu onche. 5 Dangalila lidamulika kumdima wala mdima siudatimike. 6 Padali ndi muntu uyu wadatumidwa kuchokela kwa Mulungu iyo jina lake wadi Yohana. 7 Wadaja ngati shahidi kushuhududi kuhusu lija dangalila kuti onche akoze kuamini kupitila iye. 8 Yohana siwadali dangalila lakweli ambayo washuhudie kuhusu lija dangalila. 9 Limenelo lidali dangalila lakwele ambayo idali imoja kupitila jiko lao kumtila dangalila kila mmoji. 10 Wadali katika jiko ndi jiko lidakonjedwa kupitila iye ndi jiko silimdajiwe. 11 Wadaja kwa vinthu vake, ndi kwa wanthu wake sii amlandile. 12 Ila kwa anyiwaja ambili yao adamlandila amba adaliamini jina lake kwa anyiao adapacha malinga yakukala wana Amulungu. 13 Ambao adabadwa, osati kwa mwazi wala kwa chikondi cha awili wala kwa chikondi cho munthu ila kwa Mulungu mwene. 14 Nalo mau lidachitika tupi ndi adalama mmitima mwatu, tawona ulemelo wake ulemelo ngati wamunthu yoka wapayoka uyo wadaga kuchokela kwa Ambuye wajala chimwemwe ndi kweli. 15 Yohana wadamshuhudia kuhusu iye ndi wakukweza sauti wadakamba, "uyu ndiye ambaye nidakamba nkhani zake nidakaka yuja siwaje pambuyo panga ndi wamkulukwiko ine kwa kifuko wakala kabla yanga." 16 Pakuti kuchokela kupitila kukamilika kwake ife tanche talandila bure kipawa pambuyo cha kipawa. 17 Pakuti lamulo lidapelekedwa kupitila Musa chimwemwe yaliyonche, muntu yote ambaye Mulungu wali katika chifua cha mbuye Yesu Kristo. 18 Palibe mwanadamu uyu wamuona Mulungu nyango yaliyonche yoka ambae ndi Mulungu wali katika chifua cha Ambuye amdita iye wajiwike. 19 Ni uunde ushuhuda ya Yohana nyengo makuhani ndimala mi adatumidwa kwake ndi Wayahudi kumfuncha, "iwe ndi yani?" 20 Bila kusitasita ndi siwadakane, ila wadayankha, ine osati Kristo. 21 Ila adamkambilka, "iwe ndiyani, ili kuti nikupache niyankho ilo atituma?" Jishuhudie iwe mwene. 22 Kwa chimwecho adamfuncha, kwaiyo iwendi yani? Chipano. Iwendi Eliya wadakamba ine osati. 23 Adakamba, iwe ndi nabii? wadayankha osati. Wadakamba, "inendi sauti yake walita kunyikani" 24 Nampho kudali ndi wanthu atumidwa paja kuchoka kwa Mafarisayo. Adamfuncha ndi kukamba, 25 "ndande yanji ubatiza basi ngati iwe osati Mkristo wa Eliya wala nabii?" 26 Yohana wadayankha wadakamba nibatiza kwa maji ata chimwecho pakati panu waima munthu uyu simusiwa. 27 Uyu nda uyo wadaja pambuyu paunga! Ine sinistahili lulegeza chingwe va viatu vake. 28 Vinthu ivi vidachichika kume Kubethania, kung'ambo ya Yordani pamalo ambapo Yohana wamabatiza. 29 Siku lidachata Yohana wadamuona Yesu niwaja kwa kurake penya mwana mbelele wa Mulungu waitenga dhambi ya pajiko. 30 Uyu ndo uyo wakamba nkhani zake nikakamba, "uyu siwaje kumbuyo kwanga ndi wamukuru kuliko ine pakuti wadali kabla yanga. 31 Sinidamjiwe iye nampho idachitika chimwecho ili kuti wavunukulidwa Israeli, kuti nidaja nidabiza kwamaji." 32 Yohana wadashuhudia wadaopna roho niichika kuchoka kumwamba mfano wa dau nchi ikakala kumwamba kwake. 33 Ine sinidamjiwe nampho iye wadaitumaini nibatize kwa maji wadanikambila, "yuja ambayo swane Roho Mtakatifu. 34 Naona ndi nashuhudia kuti uyu ndi mwana wa Mulungu." 35 Tena siku litachata Yohana wadali waima pamoji ndi opuzila wake awili. 36 Adamuona Yesu niwaenda ndi Yohana wadakamba "penye mwana wambelele wa Mulungu." 37 Opuzila awili adamvela Yohana wamakamba adamchata Yesu. 38 Tena Yesu wadang'anamuka ndi kuwaona opuzila waja namchata adamkambila mfuna chiani yankha, "Rabbi, (chifuko chake apuzisi alamakuti?)" 39 Adamkambila, majani ndi muone potela adapita ndi kupaona pamalo ayapo wadali wamalama, adakala pamoji nae siku limene pakuti idali yapata ngati saa kumi chimwe. 40 Mmoji wanyiwaja awili anyioadamvela Yohana ni wakamba nipotela kumcha Yesu wadali ndi Andrea mbale wake Simoni Petro. 41 Wadamuona m'bale wake Simoni ndi kumkambila tampacha masihi (ambayo itafasili Kristo). 42 Adampeleka kwa Yesu wadampenya ndi kukamba iwe ndi Simoni mwana wa Yohana siutanidwe Kefa, (naana yake Petro). 43 Siku lidachata nyengo Yesu yapowadafuna kuchoka kuchita Kugallaya wadampata Filipo ndi kumkambila, "nichate ine." 44 Filipo wadali mwenyeji wa Bethasaida jiko laandiandi Petro. 45 Filipo wadampata Nathanaeli ndikumkambila jampata yuja ambayo Musa wadalemba nkhani zake kupitila sheria za wanabii Yesu mwana wa Yusufu kuchoka Kunazareti. 46 Nathanieli adamkambila "bwanchitucha bwino chikoza kuchokela Kunazarete?" Filipo wadamkambila maja ndi unione. 47 Yesu wadamuona Nathanieli niwaja kwake ndi kukamba "penya Mwisraeli kweli kwakweli osati wamtila mkati mwake!" 48 Nathanieli wadamkambila, "wanijiwa bwanji ine"? "Yesu wadayankha ndi wadanikambila Filipo siwadakutane yapo udali panchi pamtengo ndidakukambila." 49 Nathanieli wadayankha, "Rabbi, iwe umona wa Mulungu! Ndi Mflume wa Israeli!" 50 Yesu wadajibu wadamkambila chifuko nidakukambila nidakuona panchi pamtengo bwa wamini siwaone vichicho vavikwa kuliko ivi. 51 Yesu wadakukambila, "Amini Amini, nikukambilani sizione mbingu nizichakuka ndi kumwona malaika wa kweli ndi kuchika pamwamba pa mwana wa Adamu."