1 1chokonkapo nina nyamula menso yanga kumwamba nakuona muntu na ntambo yopimilako mumanja mwake. 2 2ninakamba, '' uyenda kuti?'' ndipo anakamba kuli ine, ''kupima yelusalema, kuona ukulu na utali wake.'' 3 ndipo mungeli wamene tina kambisana naye ana chokapo ndiponso mungeli winango anachoka panja kuyendo kumana na eve. 4 4mungeli wa chibili anakamba kuli eve, '' tamanga ndiponso ukambe kuli munyamata uja; kuti, 'yelusalema azankala ziko yoseguka chifukwa chakupaka kwa bantu na vibeto mukati mwake. 5 5pakuti ine-uku nikukamba kwa YEHOVA-nizankala kuli eve chipupa cha mulilo cho muchingiliza, ndiponso nizankala ulemelelo pakati pake. 6 6 nyamuka! nyamuka! tabamo muziko ya kumpoto- uku nikukamba kwa YEHOVA- pakuti na kupalanganyani monga mpepo zili 4 za mumlengalenga!- uku nikukamba kwa YEHOVA. 7 7nyamuka! tabila ku ziyoni, iwe wamene unkala na''' mwana mukazi wa babiloni! 8 YEHOVA wa makamu anani lemekeza ine na kunituma kuma yiko yamene yana ku vutisa-mwa ichi ali wonse wogwila iwe, agwila ka pakati pa linso ya MULUNGU!-pambuyo pochita ivi YEHOVA, anakamba, 9 9''ine neka niza nyamula kwanja yanga pali beve, bakapolo bao bazabapoka katundu yao.'' mwa ichi uzaziba kuti YEHOVA wa makamu anituma. 10 10imbila chisangalalo, mwana mukazi wa ziyoni, pakuti ine mwine wake nibwela kunkala pakati panu!-uku nikukamba kwa YEHOVA.'' 11 11ndiponso mayiko yakulu yaza zilumikizakuli YEHOVA musiku ija. akamba, ''ndiponso muzankala bantu banga; pakuti nizankala pakati panu,'' ndipo muzaziba kuti YEHOVA wa makamu anituma kuli imwe. 12 12pakuti YEHOVA aza tenga yuda ngati choloba ngati katundu yake yoyenela mu malo yoyela ndiponso azazisankila futi yelusalema. 13 13nkala zee, wa tupi onse, pamenso pa YEHOVA, pakuti anyamuliwa kuchoka ku malo yake yoyela!