Mutu 6

1 Mu chaka chamene mfumu Uziya anafa,ninaona ambuye alinkale pamupando wau mfumu; anali pamwamba naku kwezekewa, na nyula yake inazula mutempele. 2 Pawamba pake panali selafimi; aliyense anali nama papiko; yabili anambisa kumeso kwake, nayabili yanambisa kumendo kwake, nayabili yombulululikilako. 3 Aliyense anaitana wena nakukamba kuti, ''oyela, oyela, oyela, ni Yehova wamakamu! ziko yonse yapansi niyo zula na ulemelelo wake.'' 4 Maziko yapopepetela yananyang'anya na mau ya abo bamene banali kulila, na nyumba inazula na chusi. 5 Mwaicho nina kamba, ''soka kuli ine! pakuti naonongeka chifukwa ndine muntu wa milomo yosayela, ndipo ninkala pakati pa bantu bamilomo yosayela, chifukwa menso yanga yaona mfumu, Yehova wamakamu!'' 6 Mwaicho umozi wa selafimi ana mbululukila kuli ine; anali nayo lilasha yenze kuyaka mumnja mwake, yamene ana chosa na mbaniro kuchoka ku guwa. 7 Anagwila nacho kamwa yanga nakukamba, ''Ona , ichi chagwila milomo yako; kulakwa kwako kwachosewa, na chimo yako yaombolewa.'' 8 Ninanvela mau ya ambuye yakamba, ''ni ndani wamene nizatuma; ni ndani wamene aztiyendela ise?'' Mwaicho ninakamba, ''ndine pano, nitumeni.'' 9 Anakamba, ''yenda naku bauza aba bantu, 'nvelani, koma musa nvesesa; onani koma musa ganizila.? 10 Pangani mitima ya aba bantu kusanvesesa, na matu yabo nakusanvela, muvale meso yabo kusaona chifukwa bangaone na menso yabo, na kunvela na matu yabo, na kunvesesa na mitima zabo, naku pindamuka na kupola.'' Mwaicho nina kamba, '' ambuye, kufika liti?'' eve anayanka, 12 paka Yehova ana tuma bantu kutali, na malo onse kusoba bonkalamo. 13 Ngankale bantu bokwanila 10 basalamo,izaonogeka futi;monga kacere kapena mutengo wojubiwa na mutengo wamene wasala,mbeu yoyela ili muvikamba vake."