Mutu 29

1 Soka kuli Ariel, Ariel, malo yamene Davide anankala pilizabi chaka ndi chaka; lekani mapwando yazi nkalako mokonkana. 2 Koma niza zinguluka Arieli, ndipo ba zayamba kulila na kumvesa chisoni. Ndipo ba zankala kuli ine monga Arieli. 3 Niza kuzinguluka iwe mbali yonse ndipo niza ku bisamila iwe kuku pangila mupanda, ndipo nizaika nchito zoku ganizila za nkondo kususa iwe. 4 Uza gwesewa pansi ndipo uzakamba pamene wagwesea pansi; mau yako yazankala ya pansi kuchokela ku doti. Liwu yako iza mveka ngati muzimu wamene ukamba kuchokela pansi pa doti, ndipo kunja kwa foti yako iza kamba pangono. 5 Bantu ba mbili bamene ba mafuna iwe baku kukugwesa, ba zankala ngati muchanga wosefewaa, ndipo ba mbili ba ntota ba zankala semu vopepetewa vimene vi uluka nakupita. Vizachitika maje manje, pangono chabe. 6 Yehova wamakamu azabwela kuliimwe na chongo cha mvua, chivomezi, chongo chikulu chimpepo cholimba na mvula yakaleza, ndipo nakuyaka kwa mulilo washoka. 7 Zidzakhala ngati loto, masomphenya a usiku: Gulu lalikulu la mitundu yonse lidzamenyana ndi Arieli ndi malo ake achitetezo. Iwo adzamuukira ndi malinga ake kuti amuthamange. 8 Zidzakhala ngati munthu wanjala alota kuti akudya, koma akadzuka, m'mimba mwake mulibe kanthu. Zidzakhala ngati munthu waludzu atalota kuti akumwa, koma iye podzuka, akukomoka, ndi ludzu lake losatha. Inde, chomwechonso chiwerengero cha mayiko omwe adzamenyane ndi Phiri la Ziyoni. 9 Dabwani mweka ndipo dabwani; kalani mpofu mweka nakunkala ba mpofu! nkalani bokolewa, noti na vinyo; zezeleka, noti na moba. 10 Pakuti Yehova atila muzimu wake pali iwe muimu wogona tulo maningi. Anavala menso, aneneti, na winikila mitu zanu, nabo ona. 11 Chivumbuluso chonse chankala kwa iwe mau amu buku yamene siyana seguliwe naku pasiwa. 12 Ngati buku ya pasiwa muntu chamenr saziba kubelenga, "Belenga ichi, äkamba kuti, "Siniza belenga." 13 Ambuye bana kamba kuti, Äba bantu ba bwela pafupi naine na makamwa na ulemu pa milomo zabo, koma mitima yabo ili kutali na ine, ulemu wamene ba nipasa ni malamulo ya bantu yamene ba napunzila. 14 Mwaicho, yangana, niza piliza kuchita chintu chodabiwsa pakati pa aba bantu, chodabisa pacho dabwisa, nzelu za bantu babo banzelu baza sila, naku nkala nacho chizibiso. 15 Soka kuli benve bamene ba biisa ma pulani yochokela kuli Yehova; ndipo na vamene bachita vili mumudima. ba kamba, "Nindani amene atiyangana, niba ndani bamene batizïba? 16 Upindamula vintu kuchokela pa mwamba na pansi kansi bowumba doti banga lingane na doti, kuti chitnu chamene ba umba chinga kambe kuti "Sibanani bumbe ine"pa vintu vonse panga iye, Ïye sama mvesesa"? 17 Paika ntai kangono, Lebanoni aza sanduliwa munda, ndipo munda uzankala sanga. 18 Pasiku lija bamene siba mvela mumatu yabo bazanvela mau yamu buku, ndipo menso yaba mpofu yaza ona kuchokela mumudima wawu kulu. 19 Nabo botitikishiwa bazakondwela futi muli Yehova ndipo bosauka pakti pabo baza kondwela kuli oyela wa Isilayeli. 20 Boyipa bonse baza leka, nabo paya ba zasoba nabonse bamene bachita zoipa, baza chosewapo. Iye na mua apanga muntu kunkala wosusa. 21 Bamu pamuteya abo bamene bafuna chilangamo pa mulyango ndipo bogwesa pansi bolungama na boza yabo ilibe kantu. 22 Izi ndiye zamene akamba Yehova ku nyumba ya Yakobo-Yehova, amene anapulumusa Abrahamu, "Yakobo sazamvela nsoni, olo pamenso pake sipazagwa. 23 Pamene aona bana bake, nchtio ya manja yake, baza lengesa zina langa kunkala loyela. Baza lengesa kuyela zina la oyela wa Yakobo naku yimilila boyaka ba Mulungu waba Isilayeli. 24 Abo bamene ba lakwa mumuzimu baza peza kumvesesa, bodandaulo baza punzila nzelu.